Inu mai banda mukuthandiza anthu because ndalama zimene munabera amalawi. Ndalama za cash get munagulisa ndege imene bingu anagula ndalama zili kuti musakhale ochenjera apa
@thulanimpphiri6873
Iwe ndi hule chitsilu wayamba kapeni iwe wagwa nayo my vote is peter
@RobertLuka-wy9cl
Ine ngati zika ya Malawi Joyce banda Chakwera chilima asakhaleso atsogoleri amalawi moyo wawo wose ngati mukufuna Malawi akhale wabwino.
@thulanimpphiri6873
Good job❤
@user-wm5tv7on2u
Good speech i like how you Tok my best Mom, onyasidwa anyasidwe
@user-oq5rg5mz7q
Please pamene pafika malawipaaa, sizomazichemereraaa ndizithu Zaulele. Help these people to be independent not tizizichemerera ndikupereka zithu zaulele. Mai Joyce Banda you are contributing to the poverty of this country. Help these people to be independent like you not this Nonse of building nyumba. Let’s give malawi good future, don’t take advantage of these people. 😢
@khumburanimukhupa4792
Mungozitukwanisa inu aaaaa daily salu pa phwewa grace chinga akukudikilani ku mwamba mukayakhe
@AishaChipande
Best speech our beloved former president osat chopotoka mikono chija ayi
@user-gj4li2gc8o
I like the massage osalola kulolodwa kuti ndiwe osauka powerful massage
APM MY VOTE
Ife sitikufuna zaulere ayi ife tikufuna kumazidyetsa tokha tikamalima amalawi ndi anthu olimbikila panonso sitikufuna mbusa ayi takanana abusa onse avunda basi ife sitizawakhulupililanso ayi abusa mwatipusitsa iweyo Joyce Banda usamathe zamkwamwa palibe angakuvotere iweyo ayi
Boooooooon kalindo🔥🔥🔥activist mmodzi yekha
Mayi ngati mukufuna ulemu musankhe kukhala chete.
Inu mai banda mukuthandiza anthu because ndalama zimene munabera amalawi. Ndalama za cash get munagulisa ndege imene bingu anagula ndalama zili kuti musakhale ochenjera apa
Iwe ndi hule chitsilu wayamba kapeni iwe wagwa nayo my vote is peter
Ine ngati zika ya Malawi Joyce banda Chakwera chilima asakhaleso atsogoleri amalawi moyo wawo wose ngati mukufuna Malawi akhale wabwino.
Good job❤
Good speech i like how you Tok my best Mom, onyasidwa anyasidwe
Please pamene pafika malawipaaa, sizomazichemereraaa ndizithu Zaulele. Help these people to be independent not tizizichemerera ndikupereka zithu zaulele. Mai Joyce Banda you are contributing to the poverty of this country. Help these people to be independent like you not this Nonse of building nyumba. Let’s give malawi good future, don’t take advantage of these people. 😢
Mungozitukwanisa inu aaaaa daily salu pa phwewa grace chinga akukudikilani ku mwamba mukayakhe
Best speech our beloved former president osat chopotoka mikono chija ayi
I like the massage osalola kulolodwa kuti ndiwe osauka powerful massage
Ife zogawazo tatopanazo tikufuna tizipanga zanthu zolandilazo ndiye zausiruzo zimenezo
Nkhani ndiya straight iyi peter mutharika anthu amadana awa kwacha mayi atisokosere uyu anapumatu😂😂😂
APM my vote koma kalindo ekhayo akusambwanzani mayiii
Well spoken i do proud of you always mama
Allomwe kwao ndi kutukwana nanga si sukulu inavuta
Mutilakwitsa mayi, zipatseni ulemu nokha
Good speech mama❤❤❤