50 + 1 was a judgement conived by MCP and the Judges. Now the same MCP seems it as a disadvantage to win the 2025 election. So let it remain like that, God os God, Chakwela ndi u Satana wake avutika.
@user-jn9tz3li3v14 күн бұрын
Those judges. I don’t know how far they are now with their reputations. They betrayed Malawi.
@johndauya224514 күн бұрын
The only thing I blame this country is that we divided ourselves into three and we need to understand if this continues koma nde tudzavutika and will never develop
50 + 1 was a judgement conived by MCP and the Judges. Now the same MCP seems it as a disadvantage to win the 2025 election. So let it remain like that, God os God, Chakwela ndi u Satana wake avutika.
Those judges. I don’t know how far they are now with their reputations. They betrayed Malawi.
The only thing I blame this country is that we divided ourselves into three and we need to understand if this continues koma nde tudzavutika and will never develop
Anankhumwa tazikalimani mbatata tizikakugulani kwachinakanaka 😂😂😂😂😂
Good point bambo banda ❤
Ndipo ngalu ameneyi chakela azaziona wakumwamba akazamuyang'anila kumbali km ubwino wake akudziwa kt waluza kale ndiye alibe ntchito galu wamunthu chakwela
Now it's when we will know how our courts behave otherwise Nankhumwa is not fit to be a leader of opposition
Akhothi ndi omwe akupangitsa kuti a Navitcha asakhale ndi mphamvu adagulidwa ndi MCP
MCP ndigalu simuzayiwona voti Yanga .MCP rabish
Mudalankhulamo za nzarutu iyiyi yokha Mr Steve
i like this guys analysis I wonder why we don't like this channel
Apatu Steve lero wanyankhulako zanzeru sunaope chakwera
Kalanga ine .. chilichonse kulilongwe ?? Ma boma enawa tizingodya nyika emweyo mcp kuzuza
Agalu awa angotinamiza ife amalawi akut ona kupusa kwambiri, ndimadabwa nawo ife amalawi ife osauka koma timankhala ndimantha kwambiri ndichifukwa ationelera agaluwa
Anankumwa ngati zavuta kumeneko vomerezani bwerani kuno ku South Africa tizizagwira maganyuwa bro bola musinthe Malo ovutikira
Kkkkkkkkkk
Nankhumwa ndiwosokoneza kwambiri,
Timvele nawo
😂😂😂😂😂 Nankhumwa tapezani zochita zina
Mmmmm malawi for sale
Chilichonse kulilongwe bwanji zigowozonse zizima pazokha aliyense azipangazaka kumpoto pakat kumwera ndikumawa asativutisepo awa
Wamkulu mutu galu amulume Nakhumwa alibe manyazi nzeru mmutu zikuoneka kuti nzopelewera
Esh
Mwana achepa nazo uyu
Passport ku lilongwe ID ku lilongwe Madera ena zero??? Boma la kuba
Steve ...gud explanation
Gwedegwede ya athu awili okha bas chiyambilen program iyi athu muli ndi zibwana muzi ntchitomu bas
Makamaka Joyce banda akundi nyatsa kwambili anawononga dziko komaso wakambilana ndi chakwela kuti akhalangati akupanga dzake lilibodza akudziwakuti kwmwela chakwela sanga patse ndiye akufuna ku pombonedza dpp kuti agawane mavot kumwela pakat akudziwa kut mcp niyawo chenjelani ni Joyce banda chonde athu akumwela chotsani akubawa panpando Joyce chakwela chilima please amalawi asawela Joyce banda wakuba ameneyu mayi okuba ngati ameneyu sinamuwone pamoyo wanga bingu anasiya ndege komaso dziko lamalawi lilibwino kwambili anabwela mu dzaka dziwili dzokha analemela modetsakhawa galuyu Wa mayi anabwela Peter anakudza lelo mukut mupangetso kapeni mwaononga kale mu tsiyeni Peter muthalika akodzeso ngati kale unu mudziononga iye azikodza monga chitsilu chanu Peter niwophudzila kwambili osati inu ayi
Ine ndikadakonda kuti zibwelere chikare chipani chilichose chizaime pa chokha
A DPP mukatenga boma zanu zopanda tsankho zija musiye. Akakamira boma. Pangani za federal tidzipanga zathu kumwera kuno. Awonso adzipanga zawo.
Zoonad kwambiri brother
Anthu awa ali ndi anthu ambiri koma akawina sasamala anthu awo
@@user-lc3sw8iz2g Koma zinthu zimakhala zotsika koopsa ndipo njala amathesa zedi
Court la ku malawi siliziwa kuweruza chilungamo
That is politics in malawi that's why malawi is poor country because they don't know how they can do to prove our country
Trash