Chakuba ichi chinakumwa amakhala ngati wa DPP koma ali wa mcp ali ngati chiompha nkhanga chomwecho chimangonyosola nyama kumangotaya osanya kungophera njilu wachabe 😢😢😢😢
@mussamapira80111 күн бұрын
😅 President wanji opanda ma looks
@wangachindeya857711 күн бұрын
Chiomba nkhanga too much eating beware Malawi kkkj
Forming personal parties is not a solution to our development please avoid forming family parties
@BenBotolo9 күн бұрын
DPP Boma 2025😂😂😂 nakhumwa ndi gawo
@FatimaKazembe-ot1os10 күн бұрын
😂😂😂 50+1 ukuwona ngt masewera kkkk😅
@user-pj7hn2ky5j11 күн бұрын
Or atakhala ndi chizindikiro chofanana ngati dpd sangasokoneze a Malawi, anthu adzaona pomwe pali chimanga osati mbalame wagwa naye ameneyo! APM motoooooo Navicha more fire in Parliament
@user-uf4db7im7d11 күн бұрын
Izi ndi zipan zakuba sorry Malawi samalan ndithu
@user-xm3zl5cg6x11 күн бұрын
Anakhumwawotu Kaya awonesa zichani zake zimenezo iyeo sangakhaleso president ngakhale patavuta motani ndi mp akuluzaso ameneo 😂
@user-jl6sq3ph1b11 күн бұрын
PDP security forces
@LandiranJubeck11 күн бұрын
Zopanda mchere nakhumwa angakhale president 😂
@user-be3is8rc4r11 күн бұрын
Eti-eti-eti???
@gabrielben-vj2eb11 күн бұрын
Nakhumwa yemweyo 2025 more fire
@CyprianoSandalamu11 күн бұрын
Nankhumwa yomweyo kuli wawawa zili bwino zipani zose anachita kuyambisa adpp analibe ndi mp yemwe inu pitilini ndi ufulu wanu
@user-pt8wb4vw6r11 күн бұрын
Watha uyu basi
@alexsumani682311 күн бұрын
Zogwilizanatu izi ndi a mcp akufuna aisokoneze dpp akufuna anthu adzabalalike povota cholinga asadzaipeze 50 1 pasana pawo sizintheka zimenezo
@EstherPeter-cf1vf10 күн бұрын
He is not 2 late , but he is weak , even he was a leader of opposition he done nothing Zipani zonse ndizadyela , inshort
@rashidadan253311 күн бұрын
More fire Dr Namnkhumwa dziko likufuna atsogoleri achinyamata opanda matha kunena za kumtima kwawo this is our next president mufune musafune Dr chilima Dr Namnkhumwa Enock chihana,Atupele muluzi dziko lokomera tonse more 🔥
@EmercianahKasiku-en6hl11 күн бұрын
Zamchere nde zija akumakodzedwa asakudziwa adad ali pa msonkhano zija 85 yrs old Gogo kumamulimbikira kit alamulebe Anthu aulesi inu imilani inuyo lija Gogo lakula mwauponda mumafuna muzizasolora muti adadiwo akugona nfi ukalamba 😅😅😅😅 Eagle waona kale sigwira dpp kutha ngati makatani 😢
@EmercianahKasiku-en6hl11 күн бұрын
koma Malawi muntu wa 80 years akapanga chiyani
@lazaruschitsamba839411 күн бұрын
Ndie omwe sanafike Kuma 80 wa akuchita chani after kulumikizana zipani 9 komabe zakanika kufikira zomwe wa 80 yo anazifikira 😂. Mulungu akutiphunzitsa kulemekeza achikulire ,adadziwa kuti wachikulire amakhala ndimaganizo okhwima ndichifukwanso afikira zaka 80
@duncainjimmy11 күн бұрын
Mbuzi ya mano pansi Nan'khumwa..Zaka 4 ukungololera kuti boma lizizunza a Malawi bola iwe ukumatsidwa zammanja , Ndiyeno do you think kuti ndindani yemwe angakhulupilire iwe.. Musapusitse an'thu apa , Amalawi akutulukirani mapulani anu wonse ,Iwe Galu Nankhumwa pamodzi Gwape Frank Tumpale Mwenefumbo", Nonsenu ndinu a MCP up to now, Achayini akenu mukuti kuchalira kuyisokonedza Dpp mu 2025 election .. Mmm mwawuponda .Amalawi 2025 akukasamutsa Mbava zonse zomwe zili ku State House , Ndipo tikukayikako APM ..Even muzabele nkulengezanso kuti Chakwera wawina" Koma Amalawi sadzalora inu kuti muwazunzenso ×2 .Apono ndiye tidzagendanano zogendana basi
@mkhulukinyata51989 күн бұрын
Nankhumwa chifukwa amayenda ndi mcp zeru walibe chifukwa dpd ndi dpp mukuona pali kusiyana then blue kala chimozimozi ndi dpp.chipanicho abwereso kukapanga bwino bwanji nankhumwa akulimbana ndi dpp
Basitu Navitcha uja wamasuka. Moreeeee fireeeeee! APM voting yaaaaaaanga😋😋😋👍
Osokoneza uyu,ali ngati chilima,anthu woononga dziko.mozambique.
Ngati umalephela kutsutsu ku parliament ungakhale otsogoleli otani iwe muthu opanda chilungamo ngati iweyo panopa tikufuna m, tsogoleli oopa mulungu osati asatana ngati inuyo iyaa mwatitola eti
DPP pachiongolero basi wina afune asafune basi❤❤❤❤❤
APM my vote❤❤❤❤❤❤❤❤
APM my vote
A broz anga a Cemeon Phiri ulemu wanu..More fire A Nankhumwa..
Another Chichewa name for the eagle is mvundula madzi Ngati simukudziwa
😂 palibe zomuvotela mwana wachepa
Nakhumwa ndiosokoneza kwambili ndipo cholinga chawo ndichokapanga alliance ndi MCP kmbe sangazamphule kanthu,DPP more fire 🔥
Mmm
Nankhumwa,chilima, Chakwera,mapwala anu.DPP APM my vote
Papah!! mwapoilatu apa😂😂😂
Nankhumwa mutu wake suukugwira wa balalika 😂😂
😂😂😂
Apm My Vote ❤
Marawi waphweka. 😢😢😢😢
Nankhumwa angamuvotere ndani? Kavuwe_vuwe
Gulukunyinda uyu galu wangwanayo
Zose izi ndikusowa zeru
adakali ndi mkhwizi ndi DPP. why choose a name similar to DPP and the colour too. akufuna kusokoneza DPP
Dpp❤❤❤❤❤
Atupele,nankhumwa,joice Banda,ndi peter onsewo azikagawana ma vote kumwera chakwera basi kuyenda mwantendere mpaka 2030 wooo
Wacita bwino kuyambisa cipani thawi yofinyana ncipani inatha Cilima akamudelela koma atayamba anagwedeza dziko
Logo ngati security company 😂😂😂😂😂
Kutha kwa a Nankhumwa😂😂😂😂
Kungokula muthu opanda zeru mbuzi ya muthu
Kkkkkkk nakhumwa kumvesa chisaoni
Vote yanga kwa ADAD DPP more fire❤
Apa ndiye waziulula yekha kuti ndi chiomba nkhanga, chimunthu choipa mtima, chodanisa, choombanisa anthu, chamoyo oipa
Akafunse NDA ya brown mpinganjira big muyende bho Inu ndi chiwomba nkhangadi
Mumachedwa kuti kadeti wa mcp tiyeni tiwonane pa ground
hahahahahahaha...koma dzikoli.....kaaya!
Nankhumwa my vote
Anapiye angapulumuke koma 😂😂😂😂😂.Rip nankhumwa
😂😂😂😂 komadi sadya ose
Aaaa mutayeni uyoo
Amp my vote
Aaaa zopusa eti ngati ulendo simukatsegula Manda ku mudzi ndi mwayi
Anakhumwa galu kwabas
Ine gulu uyu amandibowa bwanji
wachamba uyu anguvotere ndani?
Dpp❤❤
DPP bomaaaaaa iloooooooo❤❤❤❤❤
Basi nankhumwa watha palibe achita nsanje Basi mboleche sangawine malo moti akanagwirizane niazake
Mukumana ndi Chala inu
Nankhumwa sangatsogolere dziko la Malawi akudzinyenga chabe
Nankhumwa zomwe wapanga apazi ñdichimodzimodzi kukasekula babashopu yometa mavuzu ankhumba
Iwe ife ndiye tinapita kale kwa Peter ukunama
Ziliko ku Malawi eee 😅😅😅
Wachita bwino poti watiuza kale kuti ndi eagle chiomba 😂😂😂😂😂 anankhumwa mukuchepa 😂😂😂😂😂
Eggle chimbalame yowopya anthu tose tizadibwa
Kungofuna kuononga nthawi awa Sangakhare president wa Dziko wachulutsa bodza ndikudzikonda yekha
Nankhumwa manyaka😅😅😅😅
Wachita bwino kuyambitsa chipani chake nankhumwa limenelo ndiye tsogolo
Nankhumwa ayende bwino, kanauluka kanatera.. Anatopetsa kwambiri...
Nankhumwa akutsatira mapazi a Brown mpinganjira
Chitselekwete ichi chomvetsa chison APM woyeeeeeee 1:23
Chakuba ichi chinakumwa amakhala ngati wa DPP koma ali wa mcp ali ngati chiompha nkhanga chomwecho chimangonyosola nyama kumangotaya osanya kungophera njilu wachabe 😢😢😢😢
😅 President wanji opanda ma looks
Chiomba nkhanga too much eating beware Malawi kkkj
Hot 265 we love you
Zikomo Kwambiri bwana🙏🙏
Ndizo mphavu aliyense alindifulu kuyambitss chipani Ngati akukhala mopatikizika
Angozitu mcp undercover zimatheka bwanji anthu anzeru zawo kugulitsa ufulu wao chifukwa cha ndalama a Yudasi we see u throw
Koma kummwera anthu akuvutikaa kukakomzesa ma ID and akubwezedwaa so malamulo alibe ntcito
Chiselekwete chamunthu ichi compensation chison DPP ,APM woyeeeeeeeeeeeeeee
Galu iwe ukapange ndi akubanja ako dza choomba nkhanga zakozo mbudzi
mmm koma agalu awa amatiyesa agalu
Apa ndiye mwatiojeza mpaka kungwetsa passport ayi zikomo achakwera
Apm my vote
Wayambisa chipani koma palibe chomwe akuziwa mbuzi ya muthu imeneyi
zitsiru za anthu nakhumwa nkhope mutu ngati phwala
MUKAMATI msogoleli WA CHIPANI chotsutsa Boma.chipani chake chiti
tikakumana kuseu komweo
DPP my vote Nankhumwa kagwere
Kuyambisa chipani chako wachita bwino koma zomwe mwaonesa akulu kosusa tilibe chikhulupiliro painu munkangopanga zamimba yanu osati zaanthu ife president wathu ndi bon kalindo waanthu amphawi.
Kusowa zochita osamakangotsegula Ku Manda bwanji
Pano timveno akhothi ati chani uyu ndiye wayamba chipani chake ,tikungokuonanitu
a mec inu ndiinunso zitsiru
Sangawine😅
Munthu walephela kusutsa monga iye wa opposition leader mcp kudusa moyela sangakwanise kulamula boma
Kaya zanu izo zivotani muzivutika Nokha ine kuno ku joni niripheee nikudya chicken deyire
Hot 265 umakwana
Mumthu osokoneza ngati iyeyu mkumayambitsa chipani kuti zimveke bwanji ? Adad sanalakwitse kumutulutsa ku DPP
Chilima president and nankhumwa vice president.
Forming personal parties is not a solution to our development please avoid forming family parties
DPP Boma 2025😂😂😂 nakhumwa ndi gawo
😂😂😂 50+1 ukuwona ngt masewera kkkk😅
Or atakhala ndi chizindikiro chofanana ngati dpd sangasokoneze a Malawi, anthu adzaona pomwe pali chimanga osati mbalame wagwa naye ameneyo! APM motoooooo Navicha more fire in Parliament
Izi ndi zipan zakuba sorry Malawi samalan ndithu
Anakhumwawotu Kaya awonesa zichani zake zimenezo iyeo sangakhaleso president ngakhale patavuta motani ndi mp akuluzaso ameneo 😂
PDP security forces
Zopanda mchere nakhumwa angakhale president 😂
Eti-eti-eti???
Nakhumwa yemweyo 2025 more fire
Nankhumwa yomweyo kuli wawawa zili bwino zipani zose anachita kuyambisa adpp analibe ndi mp yemwe inu pitilini ndi ufulu wanu
Watha uyu basi
Zogwilizanatu izi ndi a mcp akufuna aisokoneze dpp akufuna anthu adzabalalike povota cholinga asadzaipeze 50 1 pasana pawo sizintheka zimenezo
He is not 2 late , but he is weak , even he was a leader of opposition he done nothing Zipani zonse ndizadyela , inshort
More fire Dr Namnkhumwa dziko likufuna atsogoleri achinyamata opanda matha kunena za kumtima kwawo this is our next president mufune musafune Dr chilima Dr Namnkhumwa Enock chihana,Atupele muluzi dziko lokomera tonse more 🔥
Zamchere nde zija akumakodzedwa asakudziwa adad ali pa msonkhano zija 85 yrs old Gogo kumamulimbikira kit alamulebe Anthu aulesi inu imilani inuyo lija Gogo lakula mwauponda mumafuna muzizasolora muti adadiwo akugona nfi ukalamba 😅😅😅😅 Eagle waona kale sigwira dpp kutha ngati makatani 😢
koma Malawi muntu wa 80 years akapanga chiyani
Ndie omwe sanafike Kuma 80 wa akuchita chani after kulumikizana zipani 9 komabe zakanika kufikira zomwe wa 80 yo anazifikira 😂. Mulungu akutiphunzitsa kulemekeza achikulire ,adadziwa kuti wachikulire amakhala ndimaganizo okhwima ndichifukwanso afikira zaka 80
Mbuzi ya mano pansi Nan'khumwa..Zaka 4 ukungololera kuti boma lizizunza a Malawi bola iwe ukumatsidwa zammanja , Ndiyeno do you think kuti ndindani yemwe angakhulupilire iwe.. Musapusitse an'thu apa , Amalawi akutulukirani mapulani anu wonse ,Iwe Galu Nankhumwa pamodzi Gwape Frank Tumpale Mwenefumbo", Nonsenu ndinu a MCP up to now, Achayini akenu mukuti kuchalira kuyisokonedza Dpp mu 2025 election .. Mmm mwawuponda .Amalawi 2025 akukasamutsa Mbava zonse zomwe zili ku State House , Ndipo tikukayikako APM ..Even muzabele nkulengezanso kuti Chakwera wawina" Koma Amalawi sadzalora inu kuti muwazunzenso ×2 .Apono ndiye tidzagendanano zogendana basi
Nankhumwa chifukwa amayenda ndi mcp zeru walibe chifukwa dpd ndi dpp mukuona pali kusiyana then blue kala chimozimozi ndi dpp.chipanicho abwereso kukapanga bwino bwanji nankhumwa akulimbana ndi dpp
APM my vote
APM my vote