Perfect said but pomuika Bon Kalindo mu gulu limenelo nde mukulakwitsa Bon Kalindo ndi president wa amphawife we proud of him
@AjeliMw21 күн бұрын
Walakwisa kwambiri
@meganabigail-ye7fw21 күн бұрын
Kalindo Muchoseni akulu cz iye anapepesa kale
@NgomaRaheem22 күн бұрын
Madala mulungu akudaliseni ndi mau omwe mwawagawira anthu onse mudziko lathu la Malawi. Mwalankhula bwino mopanda manthu, ndipo anthu ngati inu ndi amene akusowekela kuti dziko lathu liphulidwe mu msinga za moto. Well done papa
@user-fm8ed7eo3i22 күн бұрын
Born kalindo anapepesa mukululukileni, koma pachiyambi anasokonekela, koma anatutumuka athu atataisa kale, koma uyuyu uyu aaaaa tayeni akufuna kusokoneza wabhaletayu ndimagalaziyu,,
@WisikiBlack-gj4gu22 күн бұрын
Very good kumeneko nde kulankhula, Auzen avesese bwino bwino anthu wa
@user-un6mw5wm3x22 күн бұрын
Aaa akulu mwapalatu pamenepo kalindo anapepesa ndipo amalankhula zonveka zonzeka mwinatso kupotsa inuyo the DC nd katundu omanga ndimalamba
@KenedyBizwick-lh8bu22 күн бұрын
Kumpoto nkwachilima ndi afod not dpp nde 50+1 mukaitengakut
Komano mukudziwa kuti Bon kalindo adapepesa kwa A Malawi pachimene chidachitikaAnd We all know that no One is perfect,Freedom fighter Mr Bon kalindo is trying His Best.
@yusufuadamu547617 күн бұрын
Congratulations Mr. That's great 💪
@user-is5dl7np9g22 күн бұрын
Sure bwana.
@ivychithyoka155113 күн бұрын
Ameneyu atisamale mambo chitsiru cha munthu kuchoka ku Zambia uko
@GraceLimani-zw7dx22 күн бұрын
The dc trusted for us
@user-xd1cm7tm7t22 күн бұрын
Malawi it's for us let's stand en fight for our rights we nid to make malawi better dats it guys malawi yapoila hvy
@YakiKandeu20 күн бұрын
Awa ndi a DPP. akumva kuwawa mmene anachoseledwa muboma ndipo simuzawina wina even come 2025
@JacobKapange21 күн бұрын
Mwalankhula bwino koma koma pomutchula boni kalindo mwalakwitsa kozi iye anabwera poela nkupepesa ntundu wa amalawi ndipo amalawi anamukhululukila nchifukwa mukuona kut akalindo akalankhula amalawi akumawamvela ndi chidwi end next time osazanyozaso kalindo
@user-ve4yl1gq8e21 күн бұрын
Bon kalindo yekhayo, muchotsemoni abale.
@user-jw5rx9ze8k21 күн бұрын
Nice speech but kalindo anapepesa, so let's fight together
@andrewnjawala21 күн бұрын
Komano Bon kalindo as omenyera ufulu sakuyenera kuimilira chipani komano aziyima pa choonadi . Kalindo is the last man standing indeed. Ndangokonza pa Bon kalindo kuti aime poyera ndikulowa DPP/UDF mm ndizomwetu Mtambo wathela zolowa chipani
@duncainjimmy22 күн бұрын
Mdala uyu kwamuvuta mkunvetsetsa born kalindo amadzudzula ndipo sakunama born kalindo
@user-vh1cq5gs5u21 күн бұрын
Bon kalindooooooo
@user-zq5ob7xz4l22 күн бұрын
Muthu mulala wayowoya 200 %
@sparkdymon342918 күн бұрын
Kulakhula mwanzeru
@IsaiahPaul-xf3jg16 күн бұрын
Amen
@chipi89221 күн бұрын
Kutokota kwabwino kwambli big man
@IMEDISHAMILA21 күн бұрын
Zingayambe kuyiwalika
@GolaMwanza-oi3oj22 күн бұрын
Yes your right but only kalindo Leave him he is innocent man
@DONNEXKhama-bk1gy20 күн бұрын
Tangolankhulani zoti mzapange mkawina zanzeru please 25yrs Mndale koma zaziii
@timothymhone234022 күн бұрын
Eti ayise
@Mike-du7zt21 күн бұрын
Koma kalindo anapepesa
@joicemumba360821 күн бұрын
A Malawi tisamakhare anthu oyiwara tiyeni tiphunzire achina mtambo anatipusitsa nde achinyamata osamalora zopusa ayi
@PhillipAcquaron21 күн бұрын
Mulungu si Jacob a ziona asiyeni atase amenewo adzaithawa malawi
@GraceLimani-zw7dx22 күн бұрын
Please abwana mwayankhula bwino komano zolimbana ndi kalindo ayi kalindo ndi womenyera ufulu mwachilungamo ndipo akumenyera ufulu wa anthu osauka
@user-ml4bl2ll2g21 күн бұрын
Mau amphavu kwambiri dziko Lili paminga
@TimothyBelo22 күн бұрын
Kalindo sakupanga nawo zopusa
@Imrandaniel68321 күн бұрын
Auzeni mwina ayiwala kwatenga ngati amalawi ndi opusa auzeni akumbukile
@RobertLuka-wy9cl22 күн бұрын
Kkkk kkk kk
@user-xi4pi9qy4l3 күн бұрын
Akalindo anapepesatu nde mwaiwalatu adala bwanji mwayaka mototu
Mdala iwey according to your speech tikuziwa kut ndiwazipani ziwiri watchulazo km born kalindo musiye pliz leave that Guy alone pliz,fundo zako ndizabwn ndithu km panga zako
@WilfredMathews-yl6ij20 күн бұрын
KZhead yaphweka, munthu wandale kuyankhula zopepera chonchi, muzamanga mtambo, iwe ndi wa police? Kudzichemerera koma kuyankhula zopusa, paja umbuliwu ndi andale omwe eti? Tangoperekani maganizo anu osutsana ndi mtambo ndi andale koma akhale maganizo olongosoka osati zopusa ngati izi.
@Littlefair722 күн бұрын
I doubt the claiming here in that he is a seasoned and shrewd politician. Sound knows nothing other than being a blind royalists. He is a just a supporter of DPP and UDF as he voluntarily confesses herein. Cant understand what he is up to begging for DPP and UDF sympathy. He thinks he can advise Nankhumwa yet he needs advice himself. Nankhumwa will shame them by dividing the DPP vote. He understands very little about the Nankhumwa effect, talking about 'alibe ndarama zopangila' ma branch, what a warped political mindset. And praises fello tribesmen what do does he think he will succeeds from such mindset. He thinks kuyankhula bwino its about god washipping kkkkk and boot licking. The tongue can tell who what he is up to. To hell with your DPP
@user-dw9zi6bo3o16 күн бұрын
Uyu ndichitsilu kwambiri, ife ngati amalawi amaliseche akumwera sitikuwanaso iyeyu afune asafune tonse alliance iwinaso. Padziko lonse lapansi tikati zitukuko ndikumanga maziko atsogolo la mawa. Galu iweyo tanena zomwe amaliseche akumwera ndi DPP ndi UDF zomwe anachita zomwe zikupindulila amalawi lero lino kwa zaka 6 zomwe analamulira amalisewo ukuwatamawo. Kumangoyika Miyala basi ndalamazo mkumagawa kwa anthu akumwera chimenecho ndi chitukuko? Mbombela university ndalama aGalu inu adpp ndi UDF mwakhala mukutenga kwa zaka 6 zonse pa budget yaboma koma mpaka tinakuchotsani m'boma musanamange mbombela university. Sizokhazo ndizambiri ndipo iwalani zoti muzalowaso m'bale aGalu inu loko MEC chair person akatakhala mwana wa amaliseche akumwera simungawine chisankho. Anthu oipa inu kwambiri akudya anthu ndi mafupa omwe
@user-mj3ms4jt3b22 күн бұрын
😂😂😂 agalu kusekana zikundo , chakwera wako wapanga chani apart from devaluation, kukwera Kwa zinthu ndi corruption. Zogawa ndalamazo Aku Lilongwe kukasiya Mesa akumalandira ma 700 thousand pezan zina zolankhula akulu
@ZelinaKisswell22 күн бұрын
Ameneyudi ndi ofoyila sangaone anthu mmene akangulula njinga zamoto ndi mmidzi momwe. Kabaza sanayamba nthawi ya DPP. Pano mumuuze akayime mmaboda akaowone ndi njinga zamoto zingati or zakapalasa zikulowa
@joelmakwinjakambalame965222 күн бұрын
Speaker has just expressed brutality no connection to the mentioned kongoresi munthuyundi mwana pa ndale. You are not even a political man. UDF komwe ipite uzizimuka. DPP AND UDF ilipo?
@fumumdolo734117 күн бұрын
Ngulewakulu
@MecyKamtsuko-me2krКүн бұрын
Mani tangokambani zina ngati zokamba zatha siyani kulankhula koma sitepe mwalowayo palibe chomwe mupezemo boooooooooooooooooon kaliiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiidooooooooooooooo mmmm man timamukonda kwambili
@DanMhone-iw6xg9 күн бұрын
Mutha kunyoza enawo koma The Dcccc analapa ndipo he is here to stay uyu alowa UDF /Dpp pompa
@giftdulamkalenga734421 күн бұрын
Musiyen bon kalindo ndi pulezindet wa anthu osauka ndipo ndiyenkhao akulimba mtima kumenyela nkhondo amalawi
@YoxyKandawire-kj5vh21 күн бұрын
Inuyo mutu suli bwino ineyo sungandiyankhile zopusa iweyo ndalezo unapangapo chani kuchita kuzichemerera za ugalu basi
Musayelekeze kumuyipisa born kalindo we love him ❤
Bon kalindo please is only one man standing who is fighting for us bt sorry for including him in your audio but powerful speaking.
Ifeee tilipabuyo pa boni kalindo❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉
Ivemtimacona boni kalindo musa muymise kuyangura ndimundu wabwino❤❤❤❤❤we love you boni kalindo ❤❤❤❤
Ngulewakulu
Bon kalindo akudzudzula osat kusonyeza chibale ayi bon kalindo alibe mbali amapita kulikose musiyeni ndiyemwe akumatidziwitsa zobisika musiyeni bon kalindo
Ndale ndi bodza... Anthu mpwetekana🤣🤣🤣🤣🤣
This man is so insightful... His political observations and sayings are epitome of truth...
Bon kalindo anawapepetsa amalawi babaPolani moto kumbali ya Bon kalindo ngati pamutupanu Pali nzeru mugwirizanenaye kalindo ndipo Dpp imagination zisankho chifukwa cha Bon kalindo
Perfect said but pomuika Bon Kalindo mu gulu limenelo nde mukulakwitsa Bon Kalindo ndi president wa amphawife we proud of him
Walakwisa kwambiri
Kalindo Muchoseni akulu cz iye anapepesa kale
Madala mulungu akudaliseni ndi mau omwe mwawagawira anthu onse mudziko lathu la Malawi. Mwalankhula bwino mopanda manthu, ndipo anthu ngati inu ndi amene akusowekela kuti dziko lathu liphulidwe mu msinga za moto. Well done papa
Born kalindo anapepesa mukululukileni, koma pachiyambi anasokonekela, koma anatutumuka athu atataisa kale, koma uyuyu uyu aaaaa tayeni akufuna kusokoneza wabhaletayu ndimagalaziyu,,
Very good kumeneko nde kulankhula, Auzen avesese bwino bwino anthu wa
Aaa akulu mwapalatu pamenepo kalindo anapepesa ndipo amalankhula zonveka zonzeka mwinatso kupotsa inuyo the DC nd katundu omanga ndimalamba
Kumpoto nkwachilima ndi afod not dpp nde 50+1 mukaitengakut
Good message zoona
❤❤Zikomo
Nthawi yonseyi munali kuti osayankhula bwanji yankhulani zanu musiyeni Kalindo
DC msiyeni,kwinako tamva
After all a bon kalindo anapepesa komanso saliku chipani chilichonse
Zimenezo ndizakale kalindo adapepesa kale musiyeni pano ndi president wathu
Fire 🔥 my fada
Ife takhala tikunena boni kalindo ndiwamisala Bambo awa akulakhula zazelu osati za boni kalindo Zija ai koma macadet opanda zelu basi bze kuombela mmanja boni zazii
Very good 👍👍👍
Kweeee
Iyi ndimisala to the maximum. Nonse ndi ntambo mix MCP
Lankhulani Zina osati za born Kalindo mukusowa zonena ndimunthu yekhayo akufera ife Malawi osauka choti mudziwe
Well spoken but leave our president alone, Bon Kalindo doesn't have issues only fighting for the poor Malawians.
Akulu musakhale oweluza musireni mulungu
@@user-nc4vi1jt5g aaaa aaaa waweluza ndani apa? Muzachila 2025
Muwauze asatanawo anthu oipawo anankhumwa sangakhale pulezident
Komano mukudziwa kuti Bon kalindo adapepesa kwa A Malawi pachimene chidachitikaAnd We all know that no One is perfect,Freedom fighter Mr Bon kalindo is trying His Best.
Congratulations Mr. That's great 💪
Sure bwana.
Ameneyu atisamale mambo chitsiru cha munthu kuchoka ku Zambia uko
The dc trusted for us
Malawi it's for us let's stand en fight for our rights we nid to make malawi better dats it guys malawi yapoila hvy
Awa ndi a DPP. akumva kuwawa mmene anachoseledwa muboma ndipo simuzawina wina even come 2025
Mwalankhula bwino koma koma pomutchula boni kalindo mwalakwitsa kozi iye anabwera poela nkupepesa ntundu wa amalawi ndipo amalawi anamukhululukila nchifukwa mukuona kut akalindo akalankhula amalawi akumawamvela ndi chidwi end next time osazanyozaso kalindo
Bon kalindo yekhayo, muchotsemoni abale.
Nice speech but kalindo anapepesa, so let's fight together
Komano Bon kalindo as omenyera ufulu sakuyenera kuimilira chipani komano aziyima pa choonadi . Kalindo is the last man standing indeed. Ndangokonza pa Bon kalindo kuti aime poyera ndikulowa DPP/UDF mm ndizomwetu Mtambo wathela zolowa chipani
Mdala uyu kwamuvuta mkunvetsetsa born kalindo amadzudzula ndipo sakunama born kalindo
Bon kalindooooooo
Muthu mulala wayowoya 200 %
Kulakhula mwanzeru
Amen
Kutokota kwabwino kwambli big man
Zingayambe kuyiwalika
Yes your right but only kalindo Leave him he is innocent man
Tangolankhulani zoti mzapange mkawina zanzeru please 25yrs Mndale koma zaziii
Eti ayise
Koma kalindo anapepesa
A Malawi tisamakhare anthu oyiwara tiyeni tiphunzire achina mtambo anatipusitsa nde achinyamata osamalora zopusa ayi
Mulungu si Jacob a ziona asiyeni atase amenewo adzaithawa malawi
Please abwana mwayankhula bwino komano zolimbana ndi kalindo ayi kalindo ndi womenyera ufulu mwachilungamo ndipo akumenyera ufulu wa anthu osauka
Mau amphavu kwambiri dziko Lili paminga
Kalindo sakupanga nawo zopusa
Auzeni mwina ayiwala kwatenga ngati amalawi ndi opusa auzeni akumbukile
Kkkk kkk kk
Akalindo anapepesatu nde mwaiwalatu adala bwanji mwayaka mototu
Mukhale ngat akuluakulu abon kalindo anapepesa kale kmanso amanena kt alibe cipani
Nambo kweleko kkkkkk. Yakusawusya
Mumakwana bigman....chakwela and his cabinet should fired out.....agwa basi this 2025...APM boma.....
Chitsiru iwe
Uku ndiye kuyankhula mosapysatira
Timothy mtambo asawatenge Malawi ngt zitsulu, iye ndi Mc p yakeyoso adatikwana tionana pathawi yomvotayo
Aaaaaa nthawi imene ankapepesa born kalindo iyeyo Anali kuti? Ayimva kale audio yanuyi a born kalindo sakuyankhani. Nanga ukufuna achite kuwawuza anthu kuti azavotele Dpp anthu okha akuziwa kale amene azawavotela nde inuyo mungodila achimwene
Munthu wanzeru uyu
Msanawako basi sitikuvotelaniso kuno kumpoto a dpp
Osadera nkhawa Dpp ikubwereraso m,boma ndithu
No Bon Kalindo amabwera poyera ndikupepesa kuti pepani pamene enawa sanapepese ndiye he is innocent
Wa onse alliance uyu, musamuwone ngati ndiwa udf ayi, kuteroku alipa divide and rule, watch out!!
Kd akulu mwayambapo liti kuwamenyera amalawi ufulu?amalawi akuziwiranitu kt mufuna mugulidwe eeeeee mwayichera.mwachera kumwezi nkhanga zaona
Dpp
Iwe ngati ukudana ndi ka LINDO ndiye ndiwe wa M C P osati zinazi
Kkkk
DPP anthu akuba zaka6
Aribe ntchito ndipo paribe chomwe angapange
Uchisiru wanu ndiumene unakutulutsani dpp and udf ure not holy ndipo am promising yu guys simuzawina unless muzasinthe kachitidwe kanu
Komano Bon kalindo adapepesa let's forget about the past and move on together
No no no no we won't forget
Bon kalindo nd I pangolin
Iwe ndiwachamba kwambiri uzayelekeze kummanga ntambo uzaone kut kumpoto ndiziko palokha
Ntambo akuyenera kumagidwa, woipa
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤❤❤
UDF thetsani ilowe mu DPP...
Mdala iwey according to your speech tikuziwa kut ndiwazipani ziwiri watchulazo km born kalindo musiye pliz leave that Guy alone pliz,fundo zako ndizabwn ndithu km panga zako
KZhead yaphweka, munthu wandale kuyankhula zopepera chonchi, muzamanga mtambo, iwe ndi wa police? Kudzichemerera koma kuyankhula zopusa, paja umbuliwu ndi andale omwe eti? Tangoperekani maganizo anu osutsana ndi mtambo ndi andale koma akhale maganizo olongosoka osati zopusa ngati izi.
I doubt the claiming here in that he is a seasoned and shrewd politician. Sound knows nothing other than being a blind royalists. He is a just a supporter of DPP and UDF as he voluntarily confesses herein. Cant understand what he is up to begging for DPP and UDF sympathy. He thinks he can advise Nankhumwa yet he needs advice himself. Nankhumwa will shame them by dividing the DPP vote. He understands very little about the Nankhumwa effect, talking about 'alibe ndarama zopangila' ma branch, what a warped political mindset. And praises fello tribesmen what do does he think he will succeeds from such mindset. He thinks kuyankhula bwino its about god washipping kkkkk and boot licking. The tongue can tell who what he is up to. To hell with your DPP
Uyu ndichitsilu kwambiri, ife ngati amalawi amaliseche akumwera sitikuwanaso iyeyu afune asafune tonse alliance iwinaso. Padziko lonse lapansi tikati zitukuko ndikumanga maziko atsogolo la mawa. Galu iweyo tanena zomwe amaliseche akumwera ndi DPP ndi UDF zomwe anachita zomwe zikupindulila amalawi lero lino kwa zaka 6 zomwe analamulira amalisewo ukuwatamawo. Kumangoyika Miyala basi ndalamazo mkumagawa kwa anthu akumwera chimenecho ndi chitukuko? Mbombela university ndalama aGalu inu adpp ndi UDF mwakhala mukutenga kwa zaka 6 zonse pa budget yaboma koma mpaka tinakuchotsani m'boma musanamange mbombela university. Sizokhazo ndizambiri ndipo iwalani zoti muzalowaso m'bale aGalu inu loko MEC chair person akatakhala mwana wa amaliseche akumwera simungawine chisankho. Anthu oipa inu kwambiri akudya anthu ndi mafupa omwe
😂😂😂 agalu kusekana zikundo , chakwera wako wapanga chani apart from devaluation, kukwera Kwa zinthu ndi corruption. Zogawa ndalamazo Aku Lilongwe kukasiya Mesa akumalandira ma 700 thousand pezan zina zolankhula akulu
Ameneyudi ndi ofoyila sangaone anthu mmene akangulula njinga zamoto ndi mmidzi momwe. Kabaza sanayamba nthawi ya DPP. Pano mumuuze akayime mmaboda akaowone ndi njinga zamoto zingati or zakapalasa zikulowa
Speaker has just expressed brutality no connection to the mentioned kongoresi munthuyundi mwana pa ndale. You are not even a political man. UDF komwe ipite uzizimuka. DPP AND UDF ilipo?
Ngulewakulu
Mani tangokambani zina ngati zokamba zatha siyani kulankhula koma sitepe mwalowayo palibe chomwe mupezemo boooooooooooooooooon kaliiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiidooooooooooooooo mmmm man timamukonda kwambili
Mutha kunyoza enawo koma The Dcccc analapa ndipo he is here to stay uyu alowa UDF /Dpp pompa
Musiyen bon kalindo ndi pulezindet wa anthu osauka ndipo ndiyenkhao akulimba mtima kumenyela nkhondo amalawi
Inuyo mutu suli bwino ineyo sungandiyankhile zopusa iweyo ndalezo unapangapo chani kuchita kuzichemerera za ugalu basi