Nyanja yagulitsidwa ku Tanzania now anthuno kumalawikuno tikugulisidwanso ku Israel ndi MCP😢😢😢😢
@user-uc1pd1tc2x11 күн бұрын
Everything that is hidden carries some air of being sinister...
@FefieTenisha-du7ge11 күн бұрын
Iwe mzimayi joyce ndiwe osokoneza.unawatengera a Malawi ku ulamuliro wa nkhanza.
@abdulrafiquekalembo46911 күн бұрын
Joyce Banda asamadandaule, coz iyeyo ndiamene amatilozera kwa chakwera kumat ndi m'busa ndie lero astitopese ife tili ndi maso ndipo tikuona zonse zikuchitika.
@JonesChingaya-yf4gg11 күн бұрын
Amukazaona mtsogoleri akuti zina tinena koma zina ayi ndizachisisi muziwe kuti musogoleri yo alibe zeru akuziwa kuti zachisisizo ndizopanda pake anthu azeru akana ndichifukwa akunena kuti ndizazisisi paja mukuziwa kuti tili ndi atsogoleri a mbuli zaku Israeli zo sakuwuzani
@thulanimpphiri687311 күн бұрын
A Joyce Banda mwakalamba inuuuu. Punulani a Mai.
@mchipengule11 күн бұрын
Ukuyitha hot 265
@samsonmtumbati485511 күн бұрын
Mama nthawi ya Amai idatha,,,,,inu or nokha azkhare Zaka ziwiri mongogwirizira mwaruza kkkkkk musiyeni Peter or atupeli alamure Malawi
@user-yg9em7qq2v11 күн бұрын
Chabwino sindikuchiona ulamuliro wa chakwera
@user-vl5on2lj8b11 күн бұрын
I want my Job ,as the president promised me ,1000 jobs😂😂
@user-im7sc2my4w11 күн бұрын
Kodi chakwera ndi nkhumba chadzelu ndi chiti
@FrynessMoyo-to2du11 күн бұрын
Makape bwanji mukubisa zomwe zili mu mgwilizano wanu ndi Israeli? Kapana mukuwagulitsa anthuwa etill?😢😢😢😢😢😢
@user-qm1qb2jp4s11 күн бұрын
Kodi mayi Inu mesa chipani chanu munachigulitsa ku MCP inu
@user-tb6yh1kx3o10 күн бұрын
NO PAIN NO GAIN MALAW PAMALONDA MALAW 4SALE
@user-gx5ht9gm3z11 күн бұрын
Chimene akubisira ndichani
@user-dy4gc2hr5e11 күн бұрын
Boma lalephera apa, chifukwa akanayamba ntchito za ulimi kokuno ku Malawi kuti achinyamatawa adzigwila ntchito konkuno.
Akayambe zaulimi ku Mallawi kuno muwapatsa chiyani ku Malawi kuno anyamatawo 😂😂😂
@mchipengule11 күн бұрын
Wanzelu sanganyamukile dala waku Israel
@gabrielben-vj2eb11 күн бұрын
One million jobs 😢😢😢
@HanishaissahKagansa11 күн бұрын
Why not saying the agreement with Israel.....? We got friends and families there😢 Eeeeeish this is hectic 💔
@malawigeneralguide164611 күн бұрын
Mayi Joyce banda akudandaula chani poti ali mu mcp mo paja musayiwale kuti mcp imatenga nyasi. Za suleman ndizovesa chisoni ngati akuti sangaitanidwe kumukumano poti ali ndichileso nanga chilima wapita bwanji ku Tanzania pamene ali ndichileso. Kodi boma la mcp mitu yikuyenda koma mwina wose ndiopenga akupanga zinthu mopeoera wina kumulesa wina ayi useless people
@thulanimpphiri687311 күн бұрын
A Malawi tiyeni tiphuzile kuyamika 😂😂😂😂
@mchipengule11 күн бұрын
Chomwe ungayamikile apa ndichani? Chamzelu apa ndicha
Ngati saulula zomwe agwizana ku Israel, ndiye bwanji amaitana atola nkhani? Za ziii!
Ashilungamo amakhala opondelezedwa bass asule MN akwalakwila kukamba shilungamo
Nyanja yagulitsidwa ku Tanzania now anthuno kumalawikuno tikugulisidwanso ku Israel ndi MCP😢😢😢😢
Everything that is hidden carries some air of being sinister...
Iwe mzimayi joyce ndiwe osokoneza.unawatengera a Malawi ku ulamuliro wa nkhanza.
Joyce Banda asamadandaule, coz iyeyo ndiamene amatilozera kwa chakwera kumat ndi m'busa ndie lero astitopese ife tili ndi maso ndipo tikuona zonse zikuchitika.
Amukazaona mtsogoleri akuti zina tinena koma zina ayi ndizachisisi muziwe kuti musogoleri yo alibe zeru akuziwa kuti zachisisizo ndizopanda pake anthu azeru akana ndichifukwa akunena kuti ndizazisisi paja mukuziwa kuti tili ndi atsogoleri a mbuli zaku Israeli zo sakuwuzani
A Joyce Banda mwakalamba inuuuu. Punulani a Mai.
Ukuyitha hot 265
Mama nthawi ya Amai idatha,,,,,inu or nokha azkhare Zaka ziwiri mongogwirizira mwaruza kkkkkk musiyeni Peter or atupeli alamure Malawi
Chabwino sindikuchiona ulamuliro wa chakwera
I want my Job ,as the president promised me ,1000 jobs😂😂
Kodi chakwera ndi nkhumba chadzelu ndi chiti
Makape bwanji mukubisa zomwe zili mu mgwilizano wanu ndi Israeli? Kapana mukuwagulitsa anthuwa etill?😢😢😢😢😢😢
Kodi mayi Inu mesa chipani chanu munachigulitsa ku MCP inu
NO PAIN NO GAIN MALAW PAMALONDA MALAW 4SALE
Chimene akubisira ndichani
Boma lalephera apa, chifukwa akanayamba ntchito za ulimi kokuno ku Malawi kuti achinyamatawa adzigwila ntchito konkuno.
Zomwe akuti saululazo ndiye kuti ndi ukapolo umenewo,ngati ndizabwino bwanji sakuulula
Ndipo muli Zoopsa mumgwirizanowo
Akayambe zaulimi ku Mallawi kuno muwapatsa chiyani ku Malawi kuno anyamatawo 😂😂😂
Wanzelu sanganyamukile dala waku Israel
One million jobs 😢😢😢
Why not saying the agreement with Israel.....? We got friends and families there😢 Eeeeeish this is hectic 💔
Mayi Joyce banda akudandaula chani poti ali mu mcp mo paja musayiwale kuti mcp imatenga nyasi. Za suleman ndizovesa chisoni ngati akuti sangaitanidwe kumukumano poti ali ndichileso nanga chilima wapita bwanji ku Tanzania pamene ali ndichileso. Kodi boma la mcp mitu yikuyenda koma mwina wose ndiopenga akupanga zinthu mopeoera wina kumulesa wina ayi useless people
A Malawi tiyeni tiphuzile kuyamika 😂😂😂😂
Chomwe ungayamikile apa ndichani? Chamzelu apa ndicha