Azibusa okwela chikhoma mkumalalikla amakhala abodza ndaonela a president athu aku malawi, munthu olemekezeka mbusa koma wabodza, amalawi osavotela anthu a bodza ,mwaona Nokia kumalephela kumwa tea chifukwa cha kudula kwa sugar,malawi akumvetsa chisoni.
@user-te3ps3kf2t24 күн бұрын
Good comment bro your good person bro God you.
@user-rd4ft9nd8t24 күн бұрын
APM my vote 💪
@user-is5dl7np9g24 күн бұрын
I mean you are a good person bro God bless you good comment
😂😂😂😂😂😂😂 ma rubbish okhaokha Dpp siingazawineso sure mark my words
@talimilejosephmakawa496724 күн бұрын
@@talimilejosephmakawa4967 Ukunama adha uwonanso lija ndi Boma lokhazikika mnthesa njala eni nkhokwe
@user-uc1pd1tc2x24 күн бұрын
Only wicked people support the wicked
@chrischiwere727923 күн бұрын
Perfect ❤❤❤❤
@SolomonNjolomole19 күн бұрын
APM woyeeeeeee ❤❤❤❤❤
@user-uc1pd1tc2x24 күн бұрын
Komatu mau oti conservation nde mwawakondatu. Tiyeni tiziyankhula chichewachi aaaaaa🏃🏃🏃
@liki-likiladies---lilongwe696319 күн бұрын
Anthu enewa amayakhura ngati ndi wopemga kaya ndi ndarama zimene amalandira kwa chakwera kaya panopa basi winawake aziti akufuna president wa chinyamata kodi amene alipowo akuzuza a Malawi ndi wokaramba za ziiiii
@marryphili541924 күн бұрын
Fine vidios
@AcksonKamwanza24 күн бұрын
DPP woyeeeeeeee ❤❤❤❤❤❤❤❤
@user-uc1pd1tc2x24 күн бұрын
Tizingobandulanapo apa yamanja basi kwasalaku
@WilsonLimited-os1xd24 күн бұрын
Sizitheka tizavota opanda ma ID otherwise tizapha Chakwerayo
@user-uc1pd1tc2x24 күн бұрын
Ndipo chonde tigeilizane amalawawi tiyeni tikavotele adad osati chikhanila chimenechi chi chakwela bola adad ngakhale amafooka pena koma ndi muthu wachikondi ndipo akozaso zikoli mwinaso kuposa pamenepaja chifukwa waphuzila zambili ndipo akudziwa chomwe amalawawi akuchifuna ndipo Malawi asitha ndithu
@user-eh1mg3ww6d10 күн бұрын
Congress
@user-hq6dq7zr1e24 күн бұрын
Truly truly truly
@user-jc9gy9ou3v23 күн бұрын
Same applies to me, APM Vote
@VincentNyabanga-dw9uj24 күн бұрын
APM, ndi munthu okonda dziko lake la malawi, dpp bomaaaa, 2025
@user-lg6om6wr8z20 күн бұрын
Apm ❤❤
@user-oh5vs1gl4n24 күн бұрын
Nkhani zobera mavoti ndi nkhamba kamba pslibepo...Nkhani ndiyoti ovotawo asankha basi
man apo ndipakamwa koma musaiwale mwina munali amodzi mwaiwo umudyela ndalama palimbe chazelu chiomwe muthialika angapange muno ife ayi wakalamba
@mathewssiliya57424 күн бұрын
Zoona
@JusticeMitigolo24 күн бұрын
Kalimbanani ife pano tikugulitsa fodya ndi chakwera $3.11 utisokosela zimenezo mlimi agafune apm ndani amatibera fodya uja
@kingsleyhopematchaya518424 күн бұрын
Welll spoken apm my vote🔥🔥🔥
@eliffagondewe821424 күн бұрын
Ngati kuti DPP izalephele kulowa mmboma ndiye bola chipani china chizalowe koma mfitizi zichoke basi
@user-zg7iw8kq4r23 күн бұрын
Kodi amalawi mukufunanso Mutharika azakulamulireninso?amalawife tulo kwabasi ,munthuyo wakalamba basi.apume basi,poti amalawi simumachedwa kuyiwala.why him only.we've got young stars and integrity people who can carry our country forward.poti ndinu atulo muzamuvotela ameneyo.very shameful to my brethren
@OliverChimsewu24 күн бұрын
Iwe ulibe okaramba kwanu sasogorera mbumba ufuna ukambe chani iwe
@VincentSibu24 күн бұрын
Abwana tilembetsa bwanji pamene maboma ambili sizikutheka zikutheka ku lilongwe bas nde amenewo tingowasiya choncho bas zobela zawozo apange ndithu tidzawonesana pansewu kudzakhala mademo owopya kwambli abwana asiyeni atase mmene angathere
@IMEDISHAMILA24 күн бұрын
Inenso ndinaimva bwino kwambiri
@derekkolopo-ch7mb24 күн бұрын
That's true
@user-qp3gk8cj9g24 күн бұрын
Mwakhalamo m boma anzanthu nawo adyeko ndalama zamalawi dpp out sitikufunaso kuti achilbino azizakhala ndi matha
Iwe mbuzi petro ku zambia ,Mozambique, Tanzania ndi okwera kupambana ku malawi ndiye kwinako anakweza ndi chakwera? Fertiliser anakwera palipose ku uk anakweza ndi chakwera mbuzi yamunthu dpp inatha vomerezani chipani cha banja
@kingsleyhopematchaya518424 күн бұрын
Did they devalue their currency too?
@chrischiwere727923 күн бұрын
Mamuna yemwe mutu wake sugwira amayangana kwa neba than kukoza za nyumba mwako mkufoira
@SolomonNjolomole19 күн бұрын
Dpp, nthawi imeneyo,inachitaso chimozi mozi.lero,asalile😢😢😢,chimene,chilipo, anthu angowona,kuti if,ngati izi,zingachitike, what people of Malawi,as a citizen,tidzatani?
@HarrisonMwanga-xy4sc24 күн бұрын
DPP inatha isazabwereso
@user-fq3wz5dd2s24 күн бұрын
Koma ikuramuliratu uwona dikira
@VincentSibu24 күн бұрын
Peter muthalika ndi galu wakuba chitsiru racist nyani pusi nkhwele
Dpp 2025 ndiyomwe tikuyifuna zinaz tatopa nazo
Azibusa okwela chikhoma mkumalalikla amakhala abodza ndaonela a president athu aku malawi, munthu olemekezeka mbusa koma wabodza, amalawi osavotela anthu a bodza ,mwaona Nokia kumalephela kumwa tea chifukwa cha kudula kwa sugar,malawi akumvetsa chisoni.
Good comment bro your good person bro God you.
APM my vote 💪
I mean you are a good person bro God bless you good comment
APM is a good leader, no doubt about that.
Apm my vote
APM my vote
MCP tikuzatha nawo tizavota opanda ma ID, APM bomaaaaa iloooooo ❤❤❤❤
😂😂😂😂😂😂😂 ma rubbish okhaokha Dpp siingazawineso sure mark my words
@@talimilejosephmakawa4967 Ukunama adha uwonanso lija ndi Boma lokhazikika mnthesa njala eni nkhokwe
Only wicked people support the wicked
Perfect ❤❤❤❤
APM woyeeeeeee ❤❤❤❤❤
Komatu mau oti conservation nde mwawakondatu. Tiyeni tiziyankhula chichewachi aaaaaa🏃🏃🏃
Anthu enewa amayakhura ngati ndi wopemga kaya ndi ndarama zimene amalandira kwa chakwera kaya panopa basi winawake aziti akufuna president wa chinyamata kodi amene alipowo akuzuza a Malawi ndi wokaramba za ziiiii
Fine vidios
DPP woyeeeeeeee ❤❤❤❤❤❤❤❤
Tizingobandulanapo apa yamanja basi kwasalaku
Sizitheka tizavota opanda ma ID otherwise tizapha Chakwerayo
Ndipo chonde tigeilizane amalawawi tiyeni tikavotele adad osati chikhanila chimenechi chi chakwela bola adad ngakhale amafooka pena koma ndi muthu wachikondi ndipo akozaso zikoli mwinaso kuposa pamenepaja chifukwa waphuzila zambili ndipo akudziwa chomwe amalawawi akuchifuna ndipo Malawi asitha ndithu
Congress
Truly truly truly
Same applies to me, APM Vote
APM, ndi munthu okonda dziko lake la malawi, dpp bomaaaa, 2025
Apm ❤❤
Nkhani zobera mavoti ndi nkhamba kamba pslibepo...Nkhani ndiyoti ovotawo asankha basi
APM bomaaaaaaa 2025
Bro one love comment yabwino
We are indeed really tired with this government
Adad boma 2025 ❤❤❤❤❤
DPP WOYEEEE
Onyoza Peter wa mutharika mitu yawo,
MCP lpanidwe tiyeni tigwilane manja amalawi please please boma lri lipha anthu ambiri 😢
Yes
MCP useless government
Ndiyekuti nawonso nabera Joice banda. Sleeping on duty sangawine . Angopuma basi
😂😂❤
zaziii
Tikudikila inu adandi coz munatisiyatu malele
Ukuti tizibandulana ikubandule ndinjala muzimenya anzanu abwanawo zao zikuyenda kkkkkk
Alomwe kwanu kunatha asiyileniko anzanu sitikukufunani
Ukunama mulungu ndiwakutha satana achitamayazi
Chakwela zamanyi zakozo tiyambisa mkhondo
Zandale zikuphani
man apo ndipakamwa koma musaiwale mwina munali amodzi mwaiwo umudyela ndalama palimbe chazelu chiomwe muthialika angapange muno ife ayi wakalamba
Zoona
Kalimbanani ife pano tikugulitsa fodya ndi chakwera $3.11 utisokosela zimenezo mlimi agafune apm ndani amatibera fodya uja
Welll spoken apm my vote🔥🔥🔥
Ngati kuti DPP izalephele kulowa mmboma ndiye bola chipani china chizalowe koma mfitizi zichoke basi
Kodi amalawi mukufunanso Mutharika azakulamulireninso?amalawife tulo kwabasi ,munthuyo wakalamba basi.apume basi,poti amalawi simumachedwa kuyiwala.why him only.we've got young stars and integrity people who can carry our country forward.poti ndinu atulo muzamuvotela ameneyo.very shameful to my brethren
Iwe ulibe okaramba kwanu sasogorera mbumba ufuna ukambe chani iwe
Abwana tilembetsa bwanji pamene maboma ambili sizikutheka zikutheka ku lilongwe bas nde amenewo tingowasiya choncho bas zobela zawozo apange ndithu tidzawonesana pansewu kudzakhala mademo owopya kwambli abwana asiyeni atase mmene angathere
Inenso ndinaimva bwino kwambiri
That's true
Mwakhalamo m boma anzanthu nawo adyeko ndalama zamalawi dpp out sitikufunaso kuti achilbino azizakhala ndi matha
Anganga kulibe tipex pano yimene mnapanga inu wakalamba wakalamba siyilani anyamata achina namalomba awa akungofuna ndalama basi
Tiyeni a Malawi tiyambise mkhondo
It must be after election izayamba
Iwe mbuzi petro ku zambia ,Mozambique, Tanzania ndi okwera kupambana ku malawi ndiye kwinako anakweza ndi chakwera? Fertiliser anakwera palipose ku uk anakweza ndi chakwera mbuzi yamunthu dpp inatha vomerezani chipani cha banja
Did they devalue their currency too?
Mamuna yemwe mutu wake sugwira amayangana kwa neba than kukoza za nyumba mwako mkufoira
Dpp, nthawi imeneyo,inachitaso chimozi mozi.lero,asalile😢😢😢,chimene,chilipo, anthu angowona,kuti if,ngati izi,zingachitike, what people of Malawi,as a citizen,tidzatani?
DPP inatha isazabwereso
Koma ikuramuliratu uwona dikira
Peter muthalika ndi galu wakuba chitsiru racist nyani pusi nkhwele
Tilembesa bwanji olembawo akulemba kulilongwe, kokha,
These are all lies and I wonder where the TV is based
Akuti akudzala ma tower obela mavote Titan ifetu lazalo watikwana
Nonsense
Nkhaniyo nde ndiyoona tidzavote ndi chilichose not ID yokha ayi
Mcp out
Biased presentation. Don't bring your own ideas. Mwalandila zingati kodi?
Ukakhala wakuba umaonanso ngati anzakonso ngakuba
APM bomaaaaaaa 2025
Tizingobandulanapo apa yamanja basi kwasalaku