Anthu anakudalilani koma pano tili ndi boni kalindo amatimenyera nkhondo kuposaso iweyo galu iwe shame
@user-tn2qg1vs9j18 күн бұрын
Zoonad aaaa awa anali kale😅
@maxwellluciano494318 күн бұрын
Pamenepo 😂
@GodfreyFavorEliot17 күн бұрын
Bon Kalindo said amalawi siowafera
@ancientnkhata113715 күн бұрын
Mbava siku bweraa zaona chizango
@user-le9su3mt7r14 күн бұрын
TIMOTHY MTAMBO PLS STOP TO TAKE THE MALAWIAN'S AS YOU'R COWARDS/DZITSILU ZAKO ...WE ALL KNOWS THAT " AN'THU YINUYO PACHINA CHILICHONSE CHOMWE M'MAPANGA", YOU DO IT FOR YOUR STOMACHS BUT NOT THE CITIZEN'S AT ALL ..Pano ndiye tikukudziwanino agalu yinu bwino lomwe mwinanso kuposa momwe mukuzidziwira achayini akenu . Posafuna kutaya n'thawi mwina ndingonena kuri ; Ma Citizen's m'ngokwiya nanu kwambiri , Ndipo chikhulupiliro chathu mwayinoyo chinafa kuthetatu, Lerolino kukukhulupulirani inuyo bolanso kuwukhulupilira Mkango , Chenjezo ",", Musamale chifukwa ndimomwe yilili mikwiyo ya an'thu pano", Ndiye kuti mukhonza kutheta mmanja mwa anthu
Very pathetic to see somebody who ever lied to us coming again with lies as well inorder to correct our taxes again,may God help him to realize.
@blessedmichael512411 күн бұрын
Credible comrade
@SamsonMWNgwenya17 күн бұрын
Kodi galu mtambo ulipo, ndalama zangokuthera basi usatinyase. Galu iwe unatiyika mavuto bwanji😢
@jamesgama548918 күн бұрын
Munthu aliese amakhala ndi nthawi ya uyu ndiimeneija idatha chakwera siyemwe akubweletsa miliri ndi kusintha kwa nyengo mwina adayamba kuledzera a mtambo asatinamizeso
@user-px6kt8rx2p12 күн бұрын
Now i can assume that may be he used to bring forth with some good ideologies for the betterment of malawians but he couldn't penetrate thru.... My thoughts
Ine ndikumanena kuti zisilu zomwe zinapangisa kut anthu afe, ndi amanewa mpaka Pano amalawi akulilabe, anthu ake ndi amenewa.. ziyanthu zoila.. nzopanda pake or tikambilane za achina ntambo sizitithandiza.. tiyen ku 2025.. basi
@MikeMalinga-xx8ys18 күн бұрын
Ichi nchigalu ichi mwalodzedwa kale ndizima bangili zanuzo
@robertkipapa170913 күн бұрын
Koma inu kuyima u president muzawina tayimani big man
@user-vx6sv5wi1b17 күн бұрын
Piease try to be answering the questions in chichewa for the whole of us as Malawi
@roseemirymanda408317 күн бұрын
I phoned you Timothy mtambo, but upon realising that you were being recorded you dropped the call, conviction can't come in the fourth year
@amoschisisi207017 күн бұрын
Uyu ndi m'bulundi weniwenidi ndithu Tangomumvelani chichewa chikumuvutatu uyu....
Mwabweranso kuzalipanga support boma kkkkk Komatsu mtambo
@user-im4tc9qi4j15 күн бұрын
This led Malawian to this poverty and hard times.
@mavutotizora-yz3yn18 күн бұрын
This guy is as evil as msikidzi...who he think he is? Chimunthu choipa chazunzitsa amalawi ....all what is saying is shit ..listen to the way is answering muona kuti ndi munthu opusa mphenvu yeniyeni.....Ada awa will be responsible for all what we are facing now...if not us showing him then there is God who can definitely do that for our sake
@sjrecordschannel768716 күн бұрын
Aaaaaa iwe usatitengere kokatiyetsa ukuwona ngati a Malawi ndizitsilu
mwina wasiya china chake ku mademo akufuna akachitenge iyeyo akuganiza kuti akhalaso ndi molalo pansana pake zake zinapita basi azidya ndalama zona analandila pa u minister
@ChundaLackson15 күн бұрын
Atuma ngati mene amutumila Joyce banda wakuba ameneya
@YohanePatrick-lc2lq17 күн бұрын
komanso atolankhaniwo mwawayitanisa nonkha nde muwayankhe mwanzelu.
Antambo tinatopananu boza two much asaziwa ndani kuti ndinu aboma
@KinosiKameta-ud1ps16 күн бұрын
Mr ntambo if Malawian are thinking like an robot mean that your a biggest robot in malawi for being quite since tonse alayansi take the government....because so many things happen and you as a one of freedom fighter,citizen you keep quiet, where have been ? Now you come back while time is over for what?
@RhoydNyandule-qr2ug16 күн бұрын
Mayankhidwe awuyu mtambo sizinanveke bwino afuna atipusise pa mafunso onse sanayankhe monveka kuoneseratu kt ndi wa MCP sanayankhe funso Lina lokhunza zipani. Funso loti mulayimira chipani chit?
@SmilingFishingRod-zc4wx16 күн бұрын
Mbuzi iyi
@WisdomMsuku15 күн бұрын
Ngisunayambe utsayambeso tsiyaya machendako
@YohanePatrick-lc2lq17 күн бұрын
Atambo Pano sakudziwa zomwe akuchita awaa
@BrazioBauleni-sq9pu10 күн бұрын
Nzeru alibe uyuu iyaaa😊
@BatsonKadzuwa-tl3rp17 күн бұрын
heaven my foot...
@rasulmaulidi222417 күн бұрын
Ndipo atambo mulungu akuwoneni chomwe mumapaga simumaziwa koma
@0betPhiri-mp8kq14 күн бұрын
Chilango chilipo, ndipo chili pansi pompano muwerudzidwa pompano sure. God is watching everything.
@user-jw5rx9ze8k17 күн бұрын
Wawusilu uyu anthu ena amangidwapo chifukwa Cha ma demonstration koma iye kungikhala chete kumangowinelela osayankhula khandu koma akuti iyeyi ndi omenyela ufulu anthu sono now akufuna kufutfuta zibalima kuti anthu amukondeso Winiko wangidwa kambili mbili koma sanayankhulepo khandu koma Winiko amamangidwa chifukwa chowafunila anthu za bwino lelo akufuna kupusisa anthu powona kuti nthawi ya ma vote ikubwela ndi pomwe akubwela poyela uyu ndi Galu kwambili chikulupililo pa Atambo anthu anasiya kale. Chomwe ndiyankhule pano Amtambo muve anthu ovutikafe siyife makasu anu oti mukalima kukolola munayiwalaso makasuwo ndiye ife zotipepelesa tatopa nadzo koma ulendo wina dziko lizakutembenukilani agalu inu
Anthu anakudalilani koma pano tili ndi boni kalindo amatimenyera nkhondo kuposaso iweyo galu iwe shame
Zoonad aaaa awa anali kale😅
Pamenepo 😂
Bon Kalindo said amalawi siowafera
Mbava siku bweraa zaona chizango
TIMOTHY MTAMBO PLS STOP TO TAKE THE MALAWIAN'S AS YOU'R COWARDS/DZITSILU ZAKO ...WE ALL KNOWS THAT " AN'THU YINUYO PACHINA CHILICHONSE CHOMWE M'MAPANGA", YOU DO IT FOR YOUR STOMACHS BUT NOT THE CITIZEN'S AT ALL ..Pano ndiye tikukudziwanino agalu yinu bwino lomwe mwinanso kuposa momwe mukuzidziwira achayini akenu . Posafuna kutaya n'thawi mwina ndingonena kuri ; Ma Citizen's m'ngokwiya nanu kwambiri , Ndipo chikhulupiliro chathu mwayinoyo chinafa kuthetatu, Lerolino kukukhulupulirani inuyo bolanso kuwukhulupilira Mkango , Chenjezo ",", Musamale chifukwa ndimomwe yilili mikwiyo ya an'thu pano", Ndiye kuti mukhonza kutheta mmanja mwa anthu
Malawians are wise enough to be fooled by you.😅😅😅
Aise ntambo osatenga ngat dzikoli ndilako ayi, amalawi adutsa mavuto azaoneni chifukwa chaiweyo, zimenezo izikauza akubanja kwako
that's true bra
Iwe wabodza
Boza lachani pathako pako serious
Otumidwa ndi MCP awa kuti alumile kumbuyo pochepesa mavoti a DPP awa. Anthutu akuyiopa DPP osati masewera.Tizipani/ma pressure group onsewa akupanga za Adad basi. MUSAUVER🔥🔥🔥DPP ndi 🔥🔥
0
Mcp send you to get more vote😂😂😂😂😂
Ase this time around DPP singawinenso siyani kulota
Aaaaaa, chomwe ndatola apa, ndimafunso atolankhani basi. Koma ofunsidwawo palibechomwe ayankha chanzeru. Olomutanfusa .mwana wapabere akuuzani kuti palibechomwe chanveka. Mudaziwotchera cv nokha
Mtambo machende ako
I support your comment with one packet of sugar
Zoona big ndi munthu opusa Mtambo
You have my vote mister
Mukuona ngati ndife zitsiru..Malawi mwaipangira chani? muzitinyasa..Mwatilira
Anakakhala unduna sanawachotse sakanabwera kuzalankhura awa
And we are not sure if there will be any wise person person who will follow you again during your next film shoot Mr. Drama man😂😂😂😂😂
Drama man indeed
Ife wachilungamo tikudziwa Bon kalindo
Ndipamene anatuluka chaka choyamba ndi kuyamba kuyakhula
NKHUMBA YA MUNTHU IYI HE USED AS A TOILET PAPER 😂🎉😅
Munatibweletsera mavuto inu
Munali m'bomamo munali ziiii ,pano akuchosan muli nyoo nyoo nyoo mxm
GALU kwabas ameneyu mxiuh
People u are talking on my behalf kkkk
Mr m'tambo sitikuksowani or pang'ono kamenyereni ufuru banya ranu osati a marawi apo ayi uzingopemphera kuti mulungu azikukhurulukira chifukwatu ndiye ukuzuzisa athu
Peace and unity,,,,,,zauchitsilu! Boni kalindo wakhala akumangidwa pa nkhani za ndale chifukwa chakuti akumenyela ufulu wa anthu osauka iweyo nthawi imeneyo udatani kulimbana ndi boma kut Peace and unity ioneke pomutulutsitsa kalindo yo? Mbava iyi!
Udalikut potuluka relo bogolo , you take Malawian for grant 🥸
Another prophet from down north, much respect comrade
Comred unatha nsuzi iwe, ife tinakutuluka kale kale pita ukamu joine nankhumwa mukaendese chipani.
Mtambo came at a critical point when Malawians have lost interest in him
Ameneyu ndi galu kwa bas fit yen yen
Uyu pansana pake ndithu
From all media stations guys you now how to ask good questions... Congratulations
Mr mtambo mukuonetsa kuti ndinu mmodzi mwa anthu adyela Kodi mukuyembeza kuti enaso akupatseni ndalama pa msana pa Osaka? Nanga mukuyembeza udindo wotani kwa amene mukwalankhulira lero lino
Ine ndili pano ngati MEC volunteer just check comments & see how much votes do you have ‼️‼️ majority we say No No
Great Kalindo
Akuziona ngati Mlungu ndi mubale wake. Awoo atumidwa asatitayise nthawi. Ntchito yao anagwila kale panopa akudyelela. Bwana kumwamba kuli Mlungu
Mtambo ndi nyan
Komano muyankha bwanji funso lakumapeto kusiya oyambirila ndiye mukamawelenga mapepalaanuo mukuyambila ku manzele kumapita kumanja ngati ndiwe wachisilamu ndipo palibe chanzeru wayankhula garu iwe
Big up!!
Adzakhumudwa 2025 apa nipang,ono adziwe zimenezo amtamboo adafulumira kulowa ndale chakwera ali pa top 1
Mtambo ndiwee galu kwabasii
he has senses actually
Wamupasa chibanzi nadi AAA ukawankhu nyengo yose iyi
Kupoto kulibe muthu opanda dzelu ngati Tambo uyu ndikazizi wakumbulundi mafuso achichewa choveka bwino timayakhaso chinyanja chomwecho bwilimakhwe
Very pathetic to see somebody who ever lied to us coming again with lies as well inorder to correct our taxes again,may God help him to realize.
Credible comrade
Kodi galu mtambo ulipo, ndalama zangokuthera basi usatinyase. Galu iwe unatiyika mavuto bwanji😢
Munthu aliese amakhala ndi nthawi ya uyu ndiimeneija idatha chakwera siyemwe akubweletsa miliri ndi kusintha kwa nyengo mwina adayamba kuledzera a mtambo asatinamizeso
Now i can assume that may be he used to bring forth with some good ideologies for the betterment of malawians but he couldn't penetrate thru.... My thoughts
Kuyankhula zimenezo chfukwa choti anakuchosa pa udindo mn mzayenda nokha mmusewu
Ine umandiwaza adha ...umayankhura zanzeru though enake akuzitenga negatively
Mwafusidwa chichewa choveka bwino ndiye mukuzayakha English yanu yothoka thoka ndiziti munalowa kalasi kuzikonda bwanji iyaaa
Palibe chanzelu unganene kwa amalawi ganyu wakanika apapa unagwilisa amalawi fuwa lamoto
Only the dull will follow you. There is nothing you can say to the wise.
Timothy unadya Ntambo pano ndiye ukuti chani? Wadyanso sikono apa koma ukubweranso kuzapusisa a Malawi zoba"
Magazi onse a anthu akufa pano chifukwa chaumphawi Ali mmanja mwako and iweyo sudzapeza ntendele chifukwa chachimenechi. Ukanakhala wanzelu ukanangokhala chete.
Avala za nkhondo atambowa akuwopyezatu a Malawi akavula za nkhondozi mwina tiva
Following with interest
Kunyasa nkhope ndi mtima omwe Galu iwe kwabas palibe angakusatire iwe pumbwa iwe chimutu ngat......
Izi ndiye zopusa izi musatinyatse ife tamangodyani ndalama anakupatsayizo ☹️☹️
Musatichedwetse man
Truly. Asatichedwetse galuyu.
Aaaaaaaah man finish ni finish mkwayi😂😂😂😂😂
Ine ndikumanena kuti zisilu zomwe zinapangisa kut anthu afe, ndi amanewa mpaka Pano amalawi akulilabe, anthu ake ndi amenewa.. ziyanthu zoila.. nzopanda pake or tikambilane za achina ntambo sizitithandiza.. tiyen ku 2025.. basi
Ichi nchigalu ichi mwalodzedwa kale ndizima bangili zanuzo
Koma inu kuyima u president muzawina tayimani big man
Piease try to be answering the questions in chichewa for the whole of us as Malawi
I phoned you Timothy mtambo, but upon realising that you were being recorded you dropped the call, conviction can't come in the fourth year
Uyu ndi m'bulundi weniwenidi ndithu Tangomumvelani chichewa chikumuvutatu uyu....
Aidziwatu democracy mtambo kuti anthu saganiza mofababa
Mwabweranso kuzalipanga support boma kkkkk Komatsu mtambo
This led Malawian to this poverty and hard times.
This guy is as evil as msikidzi...who he think he is? Chimunthu choipa chazunzitsa amalawi ....all what is saying is shit ..listen to the way is answering muona kuti ndi munthu opusa mphenvu yeniyeni.....Ada awa will be responsible for all what we are facing now...if not us showing him then there is God who can definitely do that for our sake
Aaaaaa iwe usatitengere kokatiyetsa ukuwona ngati a Malawi ndizitsilu
Antambo unatichotsa kwabwinobwino kutitengela kuyipa muti chan
iyi ndiye mbudzi yazaoneni
Ntambo palibe chomwe anfanene ndipo sitikunfunanso ife Amalawi azipita uku
kodi kusukululko umaphuzila ndale basi kukamwa kobowoka
Chakwera walowesa usiwa owawa kwambiri mmalawi ife amalwawi timadya chokudya chapasiku
Mcp izalamulila ngati chipani cha ku south africa
mwina wasiya china chake ku mademo akufuna akachitenge iyeyo akuganiza kuti akhalaso ndi molalo pansana pake zake zinapita basi azidya ndalama zona analandila pa u minister
Atuma ngati mene amutumila Joyce banda wakuba ameneya
komanso atolankhaniwo mwawayitanisa nonkha nde muwayankhe mwanzelu.
Waziwa liti kuti zithu zavuta sindiwe unatingera sitingakukhulupirire iweyo
aaaaa😂😂😂😂 ichi ndiye chani wabwela ndiwe galu
Mbuz iyi he he fooled malawi for the past 3 yrs pano ndkumabwelaso koma kumutsatilaso ameneyi ndkutaya thawi adzayende yekha ulendo uno
Mtima wako mtambo mngwa dyera.🤸🤸
Ndimbava ameneyo 😂😂
Ukuyambe kunyumba kwanu how many month remaining for elections
Asatitenge ngati ndife makape uyu akagwere ukooo😂
Funso kwa CIC., Kodi nchifukw ninji.anawachotsa unduna ngati amatha?
Uyu ndi ngalu wakumba asakunamizeni Amalawi apa akufuna kukuamizaninso Amalawi
Mr Timothy mmmmmmmmm Ayi Sana
kodi ukuona ngat ife ndiopusa kape iwe ndipo ngat ndikuyenda pamsewu uyenda wekha ndi banja lako unatigwetsera kumavuto galu iwe mutu oumawo shupit
Munthu oipa iwe ukuphesa anthu tilibe nawe function
Ndipo tchende lanu akulu ndiwe opweteketsa mtima kwina kwambiri
kodi mufuna muzi atengati atora nkhaniwo chizungu samatha mesa mafusowo akukufusani muchichewa inu mukuyankha chizungu bwanji galu iwe mtambo
Unakafuna kulankhula chidzungu unakaitana atolankhani achizungu galu iwe
Lost relevance long ago, you can full the people once but you can fool the people all the time
Munali kuti inu mwaona kuti mwaonongetsa kale dzikoli, mukuona ngati malawi uja wa 2019 mumkamuyendetsa kuti palowe agulu ulumawa sichoncho, ambuye akuoneni
Antambo tinatopananu boza two much asaziwa ndani kuti ndinu aboma
Mr ntambo if Malawian are thinking like an robot mean that your a biggest robot in malawi for being quite since tonse alayansi take the government....because so many things happen and you as a one of freedom fighter,citizen you keep quiet, where have been ? Now you come back while time is over for what?
Mayankhidwe awuyu mtambo sizinanveke bwino afuna atipusise pa mafunso onse sanayankhe monveka kuoneseratu kt ndi wa MCP sanayankhe funso Lina lokhunza zipani. Funso loti mulayimira chipani chit?
Mbuzi iyi
Ngisunayambe utsayambeso tsiyaya machendako
Atambo Pano sakudziwa zomwe akuchita awaa
Nzeru alibe uyuu iyaaa😊
heaven my foot...
Ndipo atambo mulungu akuwoneni chomwe mumapaga simumaziwa koma
Chilango chilipo, ndipo chili pansi pompano muwerudzidwa pompano sure. God is watching everything.
Wawusilu uyu anthu ena amangidwapo chifukwa Cha ma demonstration koma iye kungikhala chete kumangowinelela osayankhula khandu koma akuti iyeyi ndi omenyela ufulu anthu sono now akufuna kufutfuta zibalima kuti anthu amukondeso Winiko wangidwa kambili mbili koma sanayankhulepo khandu koma Winiko amamangidwa chifukwa chowafunila anthu za bwino lelo akufuna kupusisa anthu powona kuti nthawi ya ma vote ikubwela ndi pomwe akubwela poyela uyu ndi Galu kwambili chikulupililo pa Atambo anthu anasiya kale. Chomwe ndiyankhule pano Amtambo muve anthu ovutikafe siyife makasu anu oti mukalima kukolola munayiwalaso makasuwo ndiye ife zotipepelesa tatopa nadzo koma ulendo wina dziko lizakutembenukilani agalu inu