Dr Bakili Muluzi ndi president wakale wa dziko la Malawi🇲🇼
Пікірлер
Anyamata apa town❤
@mosesharoldngolombe8 ай бұрын
1981 bakili muluzi anaba ndalama za makad a MCP, mbava yeni yeni.
@bonjechaula85423 жыл бұрын
Wow ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@EsnatSayiwala6 күн бұрын
God bless bakili muluzi adathandiza amalawi kuwachotsa muumbuli waukulu
@fanizoabrahamchimbalanga65293 жыл бұрын
Kwambiri anatisambisa kumanso
@amisichiphiri82272 жыл бұрын
We will waiting for part 2
@lastlevel19993 жыл бұрын
FDU... NICE
@ibrahimyusufu39272 жыл бұрын
Wonderful di
@davidbulla9390 Жыл бұрын
Well done sir
@fredrickkhebozy66833 жыл бұрын
Kodi achair kuba anayambira patali eti? Mpaka kuba £6? Ndi kudzasololanso K1.9bn
@Littlefair73 жыл бұрын
Komanso kulemera pamaso pa kamuzu zizinali zocheza ayi ameneyu adzafotokoze bwino part 2 akunenayo akhatiuza kuti a Gadama ndi amzawo aja akhati mukutipheranji akuwakhoma ndi hamala iye anali kuti ????????
@franciskaponda86083 жыл бұрын
Thanks for the info. Keep it up
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
I like this man chair
@alexjeremanuel2541 Жыл бұрын
Please upload it, we are waiting
@sharifsaidi67063 жыл бұрын
Bakili ndi mbuz imoz ya president mu africa opanda vision aaah tisabise apa
Nkhani ya Matafale anthu ambiri munayimva mukuthamanga. Amene anakasuma Ku polisi kuti Matafale wamubera katundu wake anali O.G ISSA. Matafale anapita Ku shop kwake ndi marasta anzake nkukaphwanya katundu yense. Sizikugwirizana ndi Bakili Muluzi izi.
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
Ati "mfana upange resign"
@chikondimwale75173 жыл бұрын
Hahaha eyetu
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
Or pano ma school achisilamu Ali kuti? Awa akungoyankhula za mmutu mwao pano ndi ndani anaphunzirapo sukulu ya chisilamu ndipo zili kuti?
@olipamaseko2693 Жыл бұрын
Masukulu achisilamu kumalawi sukuwaziwa😂😂😂
@user-cy5ko2qw5dАй бұрын
Mbiri ya Bakili ija mwalowaso za khaza za MCP kkk
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂koma adha
@LouisjrSaka3 жыл бұрын
@@LouisjrSaka kkk koma kamuzu anamulakwira chachiku mukulu ameneyu, ofcourse a MCP anali akhaza koma kumapolako
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
@@goldencitytowerent9554 chomwe adalakwa kamuzu kwa mkulu ameneyo nchachikulu heve 🤣🤣🤣🤣
@LouisjrSaka3 жыл бұрын
Zabodza izi Bakili sanaphuzile ankagulitsa matumbi ku zomba. School anaphuzila atasankhidwa kale u president
@alankasiya73293 жыл бұрын
So You mean Bakili Muluzi anapeza scholarship yokaphunzira ma college akunja mzaka za mma 1960 ali osaphunzira? I think mbuli ndi iweyo palibe chomwe ukudziwa chokhudza Bakili Muluzi.
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
Bakili muluzi ankagwira ntchito ngati clerk wa Ku court poyambilira penipeni. Ndie ukati anali osaphunzira ukutanthauza chani. Moreover bakili muluzi anali principal wa Nansawa technical college, kamuzu banda anamusankha kukhala MP komanso nduna ya boma pa nthawi yomwe anali mphunzitsi wamkulu wa pa Nansawa technical. Ndie ukati anali mbuli ukutanthauza chani. He was even minister of education mnthawi ya kamuzu. Mwina unangomvera ma propaganda a anthu kuti bakili muluzi anali osaphunzira iwe
@danielmaluwa78963 жыл бұрын
U have been mis informed Bakili ankamphuzitsidwa school ndi Dr Ken lipenganga Ali kale president. Jce and msce anazipeza Ali kale president.
@alankasiya73293 жыл бұрын
@@alankasiya7329 kutanthauza kuti ukutsutsa kuti Bakili Muluzi sanagwire ntchito Ku khothi ngati clerk? Sanagwire ntchito ngati principal pa nansawa college? Sanapite kunja mzaka za mma 1960 kukaphunzira ma college a ku Denmark ndi ku Britain? Sanakhalepo minister of education mnthawi ya Kamuzu? Ukamati we were mis informed what do you mean? Ife tikunena zoona zenizeni zooneka ndi maso pomwe iwe ukunena zongomvera anthu za mabodza. Bakili Muluzi was even minister of portfolio mnthawi ya Kamuzu, and you think munthu angakhale minister of portfolio ali mbuli?
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
@@charlesmuyaya8839 maphunzilo amene anenedwa kuti anaphuzilawo that's what I'm against kale anthu ankamphuzila up to STD 5 nkumapeza ntchito ngakhale Aleke Banda anali minister nthawi ya kamuzu koma anali ndi jc . Ngakhale ma minister ambiri muthawi ya amuluzi anali osaphunzira. Kukhala minister sikuphunzira
Anyamata apa town❤
1981 bakili muluzi anaba ndalama za makad a MCP, mbava yeni yeni.
Wow ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
God bless bakili muluzi adathandiza amalawi kuwachotsa muumbuli waukulu
Kwambiri anatisambisa kumanso
We will waiting for part 2
FDU... NICE
Wonderful di
Well done sir
Kodi achair kuba anayambira patali eti? Mpaka kuba £6? Ndi kudzasololanso K1.9bn
Komanso kulemera pamaso pa kamuzu zizinali zocheza ayi ameneyu adzafotokoze bwino part 2 akunenayo akhatiuza kuti a Gadama ndi amzawo aja akhati mukutipheranji akuwakhoma ndi hamala iye anali kuti ????????
Thanks for the info. Keep it up
I like this man chair
Please upload it, we are waiting
Bakili ndi mbuz imoz ya president mu africa opanda vision aaah tisabise apa
zoonadi abraz.
Timakunyadilani tiphuzila zambili kuchokela kwainu
Anatiombola ,palibe analimba mtima nthawi imeneija.
Kamuzu inali mbalame
Fast part 2
Dr Muluzi /kuchitekete
APA NDe mwakwanilisaatu
Anagwetsa dziko la Malawi koposa Mafia wakuba
oky?????? zako zimenezo
kuti malawi ilowe pansi ndi bakili akuluwa amakondela zoika apa.
Following
❤❤❤❤
Nawoni osawasiya abwele poyela masatanawa
Bodza tu ili adapita ku Malosa uti???
Skype Skills
Ali ndi ana angati?
I do owe his car from 1998
Narrator sangayankhule zonse zoipa za Bakili ndi abwana ake amenewa agwira ntchito ku Bakili muluzi tv
Bakili anali wamabodza kwambiri ndi amene anapangitsa kuti dzikoli lisauke kwambiri atagulitsa ma company onse a boma ndalama ndi kunyambita
Kudzindikira kodula dziwalo
nkhani ya mcp or bakili muluzi? adha inu penapake simumakhala objective with your narration
Bakili ndi dolo
Nkhani ili apa nnja Bakili or MCP? Koma akulu awa😂😂😂😂😂😘
Monga wekha sukuona kuti zikugwirizana? The narrator akufotokoza zomwe zinachitika kuti Muluzi apange resign.
Bakili anali nduna ya Kamuzu zonse zoipa amapangira limodzi ndi Bakili sikuti Kamuzu amapha yekha anthuwa ayi
@@charlesmuyaya8839 chisiyeni amwene ndichitsiru they miss understanding amavera alipanjinga 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
zokuti anapha matafale simunanenetu amwene anakakhala wa mcp bwezi ndizoipa zomwe mutanena.
Nkhani ya Matafale anthu ambiri munayimva mukuthamanga. Amene anakasuma Ku polisi kuti Matafale wamubera katundu wake anali O.G ISSA. Matafale anapita Ku shop kwake ndi marasta anzake nkukaphwanya katundu yense. Sizikugwirizana ndi Bakili Muluzi izi.
Ati "mfana upange resign"
Hahaha eyetu
Or pano ma school achisilamu Ali kuti? Awa akungoyankhula za mmutu mwao pano ndi ndani anaphunzirapo sukulu ya chisilamu ndipo zili kuti?
Masukulu achisilamu kumalawi sukuwaziwa😂😂😂
Mbiri ya Bakili ija mwalowaso za khaza za MCP kkk
😂😂😂😂😂😂😂😂koma adha
@@LouisjrSaka kkk koma kamuzu anamulakwira chachiku mukulu ameneyu, ofcourse a MCP anali akhaza koma kumapolako
@@goldencitytowerent9554 chomwe adalakwa kamuzu kwa mkulu ameneyo nchachikulu heve 🤣🤣🤣🤣
Zabodza izi Bakili sanaphuzile ankagulitsa matumbi ku zomba. School anaphuzila atasankhidwa kale u president
So You mean Bakili Muluzi anapeza scholarship yokaphunzira ma college akunja mzaka za mma 1960 ali osaphunzira? I think mbuli ndi iweyo palibe chomwe ukudziwa chokhudza Bakili Muluzi.
Bakili muluzi ankagwira ntchito ngati clerk wa Ku court poyambilira penipeni. Ndie ukati anali osaphunzira ukutanthauza chani. Moreover bakili muluzi anali principal wa Nansawa technical college, kamuzu banda anamusankha kukhala MP komanso nduna ya boma pa nthawi yomwe anali mphunzitsi wamkulu wa pa Nansawa technical. Ndie ukati anali mbuli ukutanthauza chani. He was even minister of education mnthawi ya kamuzu. Mwina unangomvera ma propaganda a anthu kuti bakili muluzi anali osaphunzira iwe
U have been mis informed Bakili ankamphuzitsidwa school ndi Dr Ken lipenganga Ali kale president. Jce and msce anazipeza Ali kale president.
@@alankasiya7329 kutanthauza kuti ukutsutsa kuti Bakili Muluzi sanagwire ntchito Ku khothi ngati clerk? Sanagwire ntchito ngati principal pa nansawa college? Sanapite kunja mzaka za mma 1960 kukaphunzira ma college a ku Denmark ndi ku Britain? Sanakhalepo minister of education mnthawi ya Kamuzu? Ukamati we were mis informed what do you mean? Ife tikunena zoona zenizeni zooneka ndi maso pomwe iwe ukunena zongomvera anthu za mabodza. Bakili Muluzi was even minister of portfolio mnthawi ya Kamuzu, and you think munthu angakhale minister of portfolio ali mbuli?
@@charlesmuyaya8839 maphunzilo amene anenedwa kuti anaphuzilawo that's what I'm against kale anthu ankamphuzila up to STD 5 nkumapeza ntchito ngakhale Aleke Banda anali minister nthawi ya kamuzu koma anali ndi jc . Ngakhale ma minister ambiri muthawi ya amuluzi anali osaphunzira. Kukhala minister sikuphunzira
He was more worse than useless
Following