kuonera live from south Africa mumakwana more fire
@user-pl6it7zc7c13 күн бұрын
😂 zazi palibe chomwe ukukamba pamenepo 😂😂😂😂 kagwele uko
@HarryRefred4 күн бұрын
Wazipeza zitsilu Ku chiladzuluko, osakuthamangitsa?
@LovemoreSalima9 күн бұрын
Zatha nfundotu, mungobweleza za kale mumawanamiza amalawi zija. Kuatengela amalawi ku mtoso basi. Olo manyazi mulibe.
@mcsellahntv689613 күн бұрын
Pepani mayi, your time is gone. You are all failures. Now is time for DPP, UDF and AFORD. Enanu mukagwere.
@omarajibu86013 күн бұрын
Dpp uDf AFoRD my vote
@EllenLuwanika-tl5ck13 күн бұрын
Aah thawi ya Dpp inatha
@chiluzbandah8 күн бұрын
@@chiluzbandah mukunama
@EllenLuwanika-tl5ck8 күн бұрын
@@EllenLuwanika-tl5ck tiyeni tidikire
@chiluzbandah8 күн бұрын
😂😂😂Sewelo latikufelanji anthu abodza awa
@ThoccoBondo-mx7vt11 күн бұрын
Manyaka weniweni🥺🥺🥺
@sthoramexjrsa90213 күн бұрын
Palibe chanzeru mukukamba inu, Chakwera anakupeperesani kale apa Chilima wanuyo azamuvotera ndi ambuyake .kodi a Amalawife mumatitenga ngati zitsiru eti
@hmshohagshohag948313 күн бұрын
Bodza la 2019/2020 lija mwayambiranso? I don't know what you guys gonna say this time. You can't fool a Malawian again, your time is over.
@omarajibu86013 күн бұрын
Akaliati zauhule basi kuyela kogulako mbudzi yamunthu zausilu basi ndi galu wakoyo chilimayo
😂😂😂😂😂😂 so funny the take Malawian for granted. Wht is doing now is in the government mxm
@chrisschikozera727113 күн бұрын
You are very correct
@AlidiNgalande-ou7ig13 күн бұрын
Sopano apa muli muboma bwanji osapanga zosezi agalu inu
@PeterPhiri-nd6op13 күн бұрын
Hule uyu ali ndikukamwatu kobowoka kkkkk
@WitnessKambwiriКүн бұрын
Akweni yokhayi yodya katatuyi Akweni sigwira ataaaaa or pang’ono kkkkkkkkkkk!
@samsonphangire152313 күн бұрын
Patrisha kawanamidze ana ako osakhala wamkulu ngati ine mmanfesto yanun : mwapanga chani mdiwe chisiru iwe kwabasi koma ndiwe wabodza eeeeeeereee satana
Onse a ndale ndi a BODZA. DPP, UTM, MCP, e.t.c, e.t.c nga BODZA. Dziko lino likufunika lilamulidwe ndi Asirikali basi. Am tired of the Politicians. Maganizo anga.
@AngungaThatcherNgoma13 күн бұрын
Apm my vote❤❤Dpp
@WilliamMsimuko-mx7fu13 күн бұрын
Amai bwererani Kwa APM kumeneko mukuchedwako chabe
@mitochilukas917012 күн бұрын
Tsopano ngat manufesito onse mudalonjeza alipo ndindani akudya ndikugula fertilizer pa mtengo omwe mudalonjeza?Koma Mcp mukuiona bwino ubale wanu mmansomo ukuupenyetsetsa? DPP plus UDF more fire
Anthu ena anangobadwa opanda manyazi ndikuyankhula.komanso anthu ena timasowekera wisdom from God kumangosatira zilizonse.zoona anthu omwewa ndiomwe anatipusisa leronso tikuwasatilanso bac atimbwititseso?koma aliboma momwemo palibe chomwe akupanga ndiye anthu opanda uzimu akuwatsatilabe komanso adzazivoteranso zitsiluzi.
Chonde amalawi, amzanga osaononga vote kamba kokuti akukunazani ndi ma ti shet kapena msalu musamale.
Huleyutu wayamba Tikuthamangitsatu ndi maduka, Usamale hure iwe.
saulo Ali muboma chipanga iye ndi chani chanzeru.
Nzeru ulibe iwe sukuona adayimisidwa ntchito kuti ngwa Kuba, ndipo wakhara asakulamura nawo, pano mwina poti akuti milandu isapitilire umboni alibe siolakwa
😢tachokani okuba inu ,mumubelenso ndani mmanyamula thumba la fertilizer paphewa palibe mwachita inu
Mmmmmm ayamba kunamanso koma amalawi tikamvera izi ndife omvetsa chisoni
Ufiti ulipodi ku Malawi 😢😢
Mmzimayi oipa manyazi alibe garu wen wen☝️
Mau amati awiri sayenda limodzi asanapangane, inuyo m'mene mumalowa mu alliance munagwirizana lero musayambe kusintha chichewa kamba koti zakuvutani. Zipitani tiyese anzanu, anzeru si inu nokha ndi a Chilima kulinso ena.
Uyu adameza memory card eeeee!!! Wayambapo Zonama zakezija.
kuonera live from south Africa mumakwana more fire
😂 zazi palibe chomwe ukukamba pamenepo 😂😂😂😂 kagwele uko
Wazipeza zitsilu Ku chiladzuluko, osakuthamangitsa?
Zatha nfundotu, mungobweleza za kale mumawanamiza amalawi zija. Kuatengela amalawi ku mtoso basi. Olo manyazi mulibe.
Pepani mayi, your time is gone. You are all failures. Now is time for DPP, UDF and AFORD. Enanu mukagwere.
Dpp uDf AFoRD my vote
Aah thawi ya Dpp inatha
@@chiluzbandah mukunama
@@EllenLuwanika-tl5ck tiyeni tidikire
😂😂😂Sewelo latikufelanji anthu abodza awa
Manyaka weniweni🥺🥺🥺
Palibe chanzeru mukukamba inu, Chakwera anakupeperesani kale apa Chilima wanuyo azamuvotera ndi ambuyake .kodi a Amalawife mumatitenga ngati zitsiru eti
Bodza la 2019/2020 lija mwayambiranso? I don't know what you guys gonna say this time. You can't fool a Malawian again, your time is over.
Akaliati zauhule basi kuyela kogulako mbudzi yamunthu zausilu basi ndi galu wakoyo chilimayo
Akuti nsomba zikaola mundengu nde kuti zonse zaona awa asatimize ayi zisilu zaathu
Akwafusa athu kuti kondi simumadya kawili akuti zimene zija zodya kawili zo zinali za UTM akuti kasala kamozi komaso athufe timangosekelela zilizonse
Chilima 2025 BOMA lanyowani
Chilima 2025 BOMA lanyowani
Wasowa chonena ameneyi.
Muthu wandale ndi satana lero akubwela ndi boza 😂😂😂
DPP woyeeeeee❤❤
Musagawe nsalu inu, gawani chimanga ndi kukwanilisa munalonjeza
Chitan manyazi akwen 😂😂😂
anthu andale ndinu oipa inu mulungu azikukhululukilani 100% tikuvutika chifukwa cha anthu andale inu
Tachionereni chikuyankhula ichochi apa manyaz bwanj isa upusa bas
Manyazi mulibe iyayi kkkkk
🎉bodza bodza bodza koma ulibe manyazi.
Takambani zina, ndiye poti amalawi ambiri tinapoila sitimadziwa chomwe timafuna boza la 2024
Anthu osowa zochita awo.
Mai opanda nzeru uyu kuwatenga amalawi ngati opusa eti
Kodi kaliati uwe ndi munthu kapena chidzukwa muudze chilima anyamule thumba lafertilizer lija ulibe nzeru chilima wakhala akunama pano angamumvere ndani mbavayo okuba ndi sattar
😂😂😂😂😂Koma mbuzi Izi akatero awanamize anthu kena
Mai opanda nzeru akuwatenga amalawi ngt zisiru,
ife pambuyo pa adadi osati onamawa ,achilimaso ndi kape anali kuti
Ukuzikolakola wekhatu 😂😂😂😂😂 muziwona katatu😢😢
Kaliat mulungu akulange😊
Zaboza zokhazokha eshii amalawi ndiyeno mukusekelela mmmmm
Amp my vote
Kukamwa konyasako mai iwe osamakayamikira amuna ako bwanji mxiii!
Manyaz mulibe mai nd chilima wanuyo kagweleni uko
Kuyankhula kwa bwanji uku mukamati munangowalawitsa anthu, kusowatu chonena uku
Mwachedwa
Mbuzi iweee
UTM my vote
Kweee is back....💪
DPP WOYEEEE!!!
Dpp tatopa nawoo apanga Chali mbili zakale
UTM my vote❤❤❤❤❤❤
Manyazi mulibe
Panyinipako hele iwe komatso nyiyamako nyiya iviyo
Mayi asazampatsabe mpando,anthu oipa akuononga dziko ndi awa
Kupepera zedi uku muuisova DPP ikulowa m'boma itchetcha afiti nonse okubanu
😂😂😂😂😂😂 so funny the take Malawian for granted. Wht is doing now is in the government mxm
You are very correct
Sopano apa muli muboma bwanji osapanga zosezi agalu inu
Hule uyu ali ndikukamwatu kobowoka kkkkk
Akweni yokhayi yodya katatuyi Akweni sigwira ataaaaa or pang’ono kkkkkkkkkkk!
Patrisha kawanamidze ana ako osakhala wamkulu ngati ine mmanfesto yanun : mwapanga chani mdiwe chisiru iwe kwabasi koma ndiwe wabodza eeeeeeereee satana
Mai oposa iwe wasowa chonena watokhuta
Chilima my vote
Olo mayi wakuyandikirayo wakhumudwa nawetu kwambiri😢😂
Palibe chamzeru chomwe mukunena mayi opusitsitsa inu, a malawi mwawatola
Aaaaaaah, musatinamizepo apa, UTM yili mu boma kale mukuchitapo chiani, za bodza basi
Onse Alliance sopano, eeeeh! Mbuzi zokhazokha.
Ulape mulungu akukhululukile
Aaaaaaaa nanunso mwasowatu zokamba wadya katatu ndani inunso anthu ndi omvesa chisoni kwambiri fertiliser wosaka mtengo mwamugula kuti mitu yanu mwaiwala nsanga nsanga
Ndinu mai ovesa chisoni mulungu sakondwera ndi boza ngati limeneli
Mbuz yosafunikira kaliat
Mayiwa ndi aboza 😂😂😂
Ingobwererani ku dpp musowatu cholankhula campaign ikubwerayi.
Nanuso pangani chipanda chilima ndinu ndani inu
Koma ndiy kuti anthu akamanama samachita manyazi kut akunama anthu akuba
Mai opanda chikondi inu mukuzanama ka chikena 😂😂😂😂 iamalawi akanali ogonabe shame
Mzimai oipa uyu za dpp unasunga zija ukabweze kwa eni aka adad mzimai oipa iwe
Chokani nonse mukulankhula mbwereranu chifukwa chilimatu paja anamuchotsa mphamvu zonse ndiye mukuona ngati angatani?chakwera ankadziwa kuti chilima simunthu wamva ndiye ndimuchotsere kaye mphamvuzo cholinga asamatsutse komanso asamapange kanthu koma akanamusiira mphamvu zonsezija ndiye pano muzikamba zimenezi zikanakhala dzomveka
MAyi. KAyimeni komwe munagwa kuja ngati zomwe munena ndizowona
owinawina SKC
Anyani Amenewa akufunika mfuti atikwanapo dzikomuno ndiboza
Padiko pako garu iwe
Mayi mulungu akukhululukileni kwambili koma ndili ndifuso kuti inu mumapemphela?
Iwe usatitenge ngati ndi chisiru wamva amalawi timazithandidza tokha sitimadadalira prezdent
Kodi mai uyu mutumu muri ubongo ndithu . Ndikukaika kwambiri .
Apm ❤
Galu uyu, ung'omboka 2024
Vuto simumaziwa kuti vice president ku malawi amachita kutumidwa ndi president, nde ngati president anamuyimisa iyeyo akanatani
Amalawi akadakhala anzelu avotere atupele muluzi..posayang'ana chipani
Onse a ndale ndi a BODZA. DPP, UTM, MCP, e.t.c, e.t.c nga BODZA. Dziko lino likufunika lilamulidwe ndi Asirikali basi. Am tired of the Politicians. Maganizo anga.
Apm my vote❤❤Dpp
Amai bwererani Kwa APM kumeneko mukuchedwako chabe
Tsopano ngat manufesito onse mudalonjeza alipo ndindani akudya ndikugula fertilizer pa mtengo omwe mudalonjeza?Koma Mcp mukuiona bwino ubale wanu mmansomo ukuupenyetsetsa? DPP plus UDF more fire
Zaziiiiii😢😢😢😢
Amai awa ndiopusa zedi alibe manyazi
😂😂😂 koma anthu andale eeesh
Zomvetsa Chisoni kwambili ndipo akamayankhura sachita manyazi
Mungosiya kupemphela mwamva
Koma, mfiti iyiih
Adadi woyeeeee
Zopusa et azakuvotera amako galu Chilima wakoyo azikalamulira kunyumba kwako demet fertilizer K4.595 alikut
Akweni mungobwelera ku DPP komkuja basi zinazi mungotukwanidwapo zamunsalu apa because we are tired of u guys ndi mabodza anuwo fotsek!!!!
Mayi opandanzelu kwambili
Malawi wake uti ameneyo😅😅
Anthu amodza inu
Chilima boma akumu nanga chilima moto buuuuu
Palibe chanzeru chomwe mwayankhula.Ulendo uno simutinamizaso. Malawi pano adazindikira ndipo zimenezi muziyankhula mnyumba mwanu nd ana anu