Kumangoti ma court, ma court ake ati??? America sinalakwise coz too much delays ma court anthu especially milandu yeni yeni osati za born kalindo anthuwa onse ngakuba chakweraso ndiye mbudzi yeni yeni.
@chitanibenito110926 күн бұрын
America ayenela kulankhula chifukwa ndi ayini ake a ndalama ,it's painful kumaona kuti akutumiza Thandie wina mkumaika mthumba make Malo mothandizila anthu Osauka
@user-te3ps3kf2t26 күн бұрын
Mbuzi ya president chakwela moyenda chinyau watikwana
@ChangeChambo26 күн бұрын
Kodi olo inuyo a kunkuyu mungalole kuti munthu amene ali ndi mbili yakuba adzibwela kunyumba kwanu kumadzacheza ndizachidziwikile kuti munthu wakuba sitimulola kubwela kunyumba kwathu
@patassonelucaszovuta343126 күн бұрын
Chakwela the fool of the foolest
@JIMMYWATHONJE26 күн бұрын
Nkhaniyo kukhotiko mpaka 4years akudikira chiyani sadalakwitse boma la America
MALAWl has destroyed because of Chakwela and his cabinet and his family , I will Happy to see this Crue are arrested , big criminals in MALAWl , We don't have court of justice here in MALAWl because all of them are under corruption of this particular government of MCP
Ma jaji athu palibe ilipo alimumbuyo ma boma lachakwela akupanga business ndichakwela ,,mukhani zakatangale
@WisikiBlack-gj4gu26 күн бұрын
Yes zoona zikanateladi kumbali,,koma chakwela inamukhudza khani ija, chifukwa mu athu akatangalewo chakwela alimo,chifukwa walupha malile kuesa kuzibisa koma ziululika zayamba kale man chakwela
@WisikiBlack-gj4gu26 күн бұрын
Zoti a Malawi adziwe nzoti milandu ku Malawi kuno ndi a ife osauka chifukwa siyimatenga nthawi kutha Ku ma court koma zandare pa nkhaniyi ayi. President wanthu afulumira ovutika tinkhara ifeyo common people. Chonde iwo a pepese
Chakwera kodi wadziwa liti kuti America ndiyokuba ndiwe galu kwambiri usazapitenso kumeneko
@ChikumbutsoJohn-rs4tt26 күн бұрын
President chakwera sadaganize polankhula kunyoza America, akukhala ngati akugwirizana ndi kuba.
@user-pv9uk6sc3w27 күн бұрын
President akuziwapo kanthu, ndithu. And kufufuza mpaka ati 4 years akufufuzabe , aaaaaah koma amene anatilozayo ndi emweyo tili ndi vuto la muwubongo makamaka akuluakulu ku ntundaku zosaenda . Ma mericans-wa ndie kuti anafufuza kale pa okha why inu mukuchedwa pa zifukwa zoti nonse ndi akuba ndie ndi zovuta kuti akuba okhaokha sangayalusane. Ndie angoona kuti anthuwa ndi amozi asatipusise tingowauza zochita bsi eyetu.
Akulu process in low yake itiyo ? Ma count athu amachedwese milandu dala ?
@robertchitsulo800627 күн бұрын
God job America 😂😂😂
@Dorah-zl9uf26 күн бұрын
In malawi we need a crismatic leader not a trained leader
@GiftMshani26 күн бұрын
🤔
@user-ce5gf4im1m26 күн бұрын
Bayana ndi wa mcp
@ChikumbutsoJohn-rs4tt26 күн бұрын
Chakwela ulibe nzelu nonse ndi mbava zokhazokha
@user-zk7jw9up6m27 күн бұрын
Chilungamo chili poelatu tisamachedwe ndikufunsana mafunso apa, chakwela walakhula zambili chifukwa waona kuti luphanga likupita kwaiye because iyeyo ali mugulu la athu 4 ayimikidwa kutuluka ku America, chakwela alimo America yangopanga manyazi kwambili
@WisikiBlack-gj4gu26 күн бұрын
Muziponya nkhani zimene zachitika.kumene osati zakale Big
@MustaphaMvula27 күн бұрын
Uyu ndiye manyi eneene
@MustafaLikaomba26 күн бұрын
America has followed its laws as quoted, the bsn is applied in America not Malawi...in Malawi they're free and relaxed BUT not America, they don't entertain those issues
@paulmakaula493726 күн бұрын
Sindikuziwa kuti anthu Andale mumayanlhula mozungulira bwanji koma nkhaniyo mukuyiona kuti ikupita apo a president akuopa kuti nkhaniyo ndiyawo
@mussamapira80127 күн бұрын
Kodi Vuto ndilakut zinthu zi ndizagulu chifukwa zinakhala za anthu watha BweZi nda police omwe akut america yachita bwino kutelo
@ChristopherBaluti27 күн бұрын
Chakwera mutu wake sugwila ntchito 😂😂😂😂mutsogoleri opoira Anthu akubvutika kwambiri no vote for 2025😂😂😂😂😂
Amalawi ku opa America dziko lopanda yankho pa lokha
@jonathanmalanda774226 күн бұрын
America yachita bwano kutelo
@petertaulo801427 күн бұрын
Kodi wakuba alindiufulu zopusa
@MustafaLikaomba26 күн бұрын
Alibe mphatso yawu president!!
@kubengovender699627 күн бұрын
Support criminal adha awa and wina akamati amuvotela😮
@johnjoachim382026 күн бұрын
Kumkuyu garu wa munthu.
@petertaulo801427 күн бұрын
Zozungulira ayi tangoyankhani mafunso komanso palibepo mbalume pamenepo ndi Street thing answer the question pls
@user-og8qm5qx8f27 күн бұрын
Makhothi ake ati,???? Ku Malawi kulibe mathoti anapangidwa Captured ndi mcp ngati injunction ya nankhumwa kutha years nde milandu zinazi anga kambe.. Tinawombera mfiti mmanja...
@eliffagondewe821426 күн бұрын
Guys ma American siwofunika kumawasekelera eya zowona amapereka mathandizo Koma amakhara ndicholinga mudzikomo pamapeto adzakupusitseni then atenge zofunazo mosavuta and we need to know dziko lirilose limene mulimikangano ma American akango yamba kulowelerapo mapeto ake dziko limalowa nkhondo mcholinga azidzapangamo ma businesses azida zankhondo president wa Malawi akadapanda kulankhulapo mukadatiso ndiwogona kwambiri
@chipanganofackison518526 күн бұрын
Chakwera is corrupt,thats why he is defending those people.
@user-yk3wc9ei5g25 күн бұрын
Dziko la Malawi limadalira kuphepmpha ku america komweko ndiye americawo awone zochita basi
@user-og4oe5yp4w26 күн бұрын
Galu waluma mbuyache kkkkkk wapenga chakwera
@user-un6qv6sj3h26 күн бұрын
Musavutike ndi kuganizaso chakwera ndi mbava.akanakhara wanzeru akanat America yandithandiza athuwa ndimbavadi
@user-zl8fl7yp8q25 күн бұрын
Chakwela ndi. Wakuba. Amange bas mboni ndine
@DylesMtenje26 күн бұрын
Makhot anthu akugwila ntchito ndi emusip
@user-hx6ly3cl8m26 күн бұрын
😂Galu wankota sakandira pachabe.les wait and see. wait
@bensonmughandira26 күн бұрын
American tsinalakwe chakwelalayo ndiye wakuba kwambili mbava dzokhadzokha sitikumu funa pamozi ndi kunkuyu achoke dpp boma 2025 tatopa komaso joice banda usiletu kunamidza athu komaso athu muchenjele Joyce anaba ndalama ya ndege anayda yekha ndiye chenjelani mudza wona mavuto ngati womwewa komasotu Joyce banda alinali ku mcp motelo idzi akupanga dala akupanga akufuna kuti dpp isawine ku mwela akufuna dpp ndi pp pakati akudziwakale kuti mcp ndiyo winawina kale chonde amalawi musapange mistake kawili Joyce ndiwo tsokonedza my name is Patrick form South Africa
@YohanePatrick-lc2lq26 күн бұрын
Makondela inu koma akanakhala azipani zina bwezi mutamanga kalekale
@user-uv7yq1fx4r26 күн бұрын
Kodi kumkuyu mmutu mwake mulimzeru?
@ShabaniKuswere26 күн бұрын
Sizikugwilizana watsala iwe
@alexmkolongo308927 күн бұрын
kumkuyunso ali limodzi muwumbsva
@JafaliAkimu-ll1bf26 күн бұрын
America sadalakwitse ,manyumba mwathu,tikaona kuti mwana wathu akuba,amasalidwa ndi abale amakolo Ake kuti asabwere kunyumba kwathu, chifukwa Cha mbiri yakuba,ndiye dziko Lili ndi anthu akuba ndye ma mericans asekere zupusazo?
@CyprianoSandalamu26 күн бұрын
Eee achita bwino pule akwiya
@user-zg9se4rw6v26 күн бұрын
Koma abaalee 😂
@violetnkhoma853527 күн бұрын
You are not honest Mr President, kutha mau chifukwa aletsa mbava kulowa dziko lawo?? Mr President mukanakhala wina mukanauza a ma court athu azifulumiza milandu osat mpaka 4yrs milandu isanathe. Munthu womvesa chisoni Chakwera.
Kumangoti ma court, ma court ake ati??? America sinalakwise coz too much delays ma court anthu especially milandu yeni yeni osati za born kalindo anthuwa onse ngakuba chakweraso ndiye mbudzi yeni yeni.
America ayenela kulankhula chifukwa ndi ayini ake a ndalama ,it's painful kumaona kuti akutumiza Thandie wina mkumaika mthumba make Malo mothandizila anthu Osauka
Mbuzi ya president chakwela moyenda chinyau watikwana
Kodi olo inuyo a kunkuyu mungalole kuti munthu amene ali ndi mbili yakuba adzibwela kunyumba kwanu kumadzacheza ndizachidziwikile kuti munthu wakuba sitimulola kubwela kunyumba kwathu
Chakwela the fool of the foolest
Nkhaniyo kukhotiko mpaka 4years akudikira chiyani sadalakwitse boma la America
Makhothi kulibe, Acb kulibe asamaname apapa ma Judge nda Mcp aweruza bwanji milandu🙌🙌
MALAWl has destroyed because of Chakwela and his cabinet and his family , I will Happy to see this Crue are arrested , big criminals in MALAWl , We don't have court of justice here in MALAWl because all of them are under corruption of this particular government of MCP
Chakwela kunkuyu chimwendo mkaka mukuzitenga ngat Madolo muli agalu enene fwesek
President wopanda manyazi ndipo mwayaluka Kuba mupaka ku dziko la eni ake mwalengeska Malawi
Pulezidenti omvetsa chisoni ndipo alibe manyazi
Chilungamo chili poyela apa abale palibe zozungulila zungulila apa ,milandu paka ifike 2025 kuma vote 🗳 chigamulo chizakhala liri?
Çhakwela ATI tiyipasemoto yakuba 😂 okalozedwa suununkha chithandizo muchipeza Kuti. AAAAAA chimozesi kukuyu 😂😂😂 mbuziyi yatisausa
Ma jaji athu palibe ilipo alimumbuyo ma boma lachakwela akupanga business ndichakwela ,,mukhani zakatangale
Yes zoona zikanateladi kumbali,,koma chakwela inamukhudza khani ija, chifukwa mu athu akatangalewo chakwela alimo,chifukwa walupha malile kuesa kuzibisa koma ziululika zayamba kale man chakwela
Zoti a Malawi adziwe nzoti milandu ku Malawi kuno ndi a ife osauka chifukwa siyimatenga nthawi kutha Ku ma court koma zandare pa nkhaniyi ayi. President wanthu afulumira ovutika tinkhara ifeyo common people. Chonde iwo a pepese
Pamafunika kt milandu yonse imene ili mmakhoti izengedwe chaka chino chisanathe coz kuzengereza kuzenga milandu ndichifukwa chake maiko ataya chikhulupirilo ndimmene tukuchitira
America sinarakwuse coz america ikutivera chison ife amarawi coz khani ikakhara ku court imachedw kt aweruze mpaka zaka zambili
chakwera ndi chitsiru zamukwana ban imeneyi chifukwa iye ndimbavanso yayikulunso
Mbava chakwela
Plezident waunsilu ameneyu
Milandu ili mokoti ,, tsono mosemuja mukoti igemulidwa liti kodi kufufuza kwake kotani
Chakwera kodi wadziwa liti kuti America ndiyokuba ndiwe galu kwambiri usazapitenso kumeneko
President chakwera sadaganize polankhula kunyoza America, akukhala ngati akugwirizana ndi kuba.
President akuziwapo kanthu, ndithu. And kufufuza mpaka ati 4 years akufufuzabe , aaaaaah koma amene anatilozayo ndi emweyo tili ndi vuto la muwubongo makamaka akuluakulu ku ntundaku zosaenda . Ma mericans-wa ndie kuti anafufuza kale pa okha why inu mukuchedwa pa zifukwa zoti nonse ndi akuba ndie ndi zovuta kuti akuba okhaokha sangayalusane. Ndie angoona kuti anthuwa ndi amozi asatipusise tingowauza zochita bsi eyetu.
Maloya ake mbavazo mese amachedwesa mulandu daladala kumaonangat amalawi ndiopusa
Mbava zokha zokha mwaonjeza kwambiri bomalimeneli ndi LA anthu okuba kwambiri zikubisana chifukwa onse ndi ambava kulibwino achoke anthu amenewa sakuthandiza mzika za amalawi
Musadabwe nazo akudziwa zochita America kalipo kalipo
Achakwera akuopa awa kuti kwatsala tchire ndikomwe kupita moto. Akudziwa kuti nayenso akachoka pampando milandu yake ikazayamba iyeyu ndi ana ake adzaletsedwanso kulowa ku America poti ndikumene amakabitsa ndalama akuwabela amalawi.
Mvuto a chakwela iwonso ndi mbava ndi chifukwa achita zimenezi
Aba zambiri ayamba kukula mtama a Malawi kkkkkkkk tiziona.
Umphawii sizinthu ayi antthu amakutukwana chifukwa chaumphawi apule ali ngati kholo tele amalawi akutukwana apule chifukwa chowayimila
Chakwela ndiwolakwa
Iiii kunkuyu ngati sudziwatu iweyo mkaka , zikhale , Richard ndiamene mukuononga dziko lathu dziwa lero
Akulu process in low yake itiyo ? Ma count athu amachedwese milandu dala ?
God job America 😂😂😂
In malawi we need a crismatic leader not a trained leader
🤔
Bayana ndi wa mcp
Chakwela ulibe nzelu nonse ndi mbava zokhazokha
Chilungamo chili poelatu tisamachedwe ndikufunsana mafunso apa, chakwela walakhula zambili chifukwa waona kuti luphanga likupita kwaiye because iyeyo ali mugulu la athu 4 ayimikidwa kutuluka ku America, chakwela alimo America yangopanga manyazi kwambili
Muziponya nkhani zimene zachitika.kumene osati zakale Big
Uyu ndiye manyi eneene
America has followed its laws as quoted, the bsn is applied in America not Malawi...in Malawi they're free and relaxed BUT not America, they don't entertain those issues
Sindikuziwa kuti anthu Andale mumayanlhula mozungulira bwanji koma nkhaniyo mukuyiona kuti ikupita apo a president akuopa kuti nkhaniyo ndiyawo
Kodi Vuto ndilakut zinthu zi ndizagulu chifukwa zinakhala za anthu watha BweZi nda police omwe akut america yachita bwino kutelo
Chakwera mutu wake sugwila ntchito 😂😂😂😂mutsogoleri opoira Anthu akubvutika kwambiri no vote for 2025😂😂😂😂😂
Mbava zokha okha izi mkuona zikuberekana iyaaa. Timakhalira kukapempha konko,. Sitikidzera mpoto ophika nsima
Chakwela is efeliaa
Dziko la malawi limadalu
Manyumba mwanga onse oganilizidwa zakuba asalowe. Yatero America. Simple
Makhotiso mukumapanga chinyengo mukudziwa kit anatigura chakwera
Chakwela nd I mbuzi ya president
Ukamamubwezera mawu munthu okuzuzula zimangowoneseratu kuti ukuvomereza kulakwakwako . Kunena zowona boma lachakwera ndirazimbava ndipo makhoti onse Akulamuliridwa ndi chakwera ndi chipanichake cha mcp. Akunkuyunso sangalankhule chirungamo chifukwanayenso ndibamva.
Wosawuka alibe mawu ,mukanakumana Kaye NDI anzanu wotsutsa boma akupatseni mayankhidwe
Chakwera ndi chitsilu amaleka kuyakhula chizungu chakwa America bwanji
Ndeakuti ma Court anthu akumalawi amatha kugwira ntchito kuposa America????😂😂😂 Koma Chakwera guys i think wapenga
Kodi nkhaniyo kumakothiko idapita liti? Koma mukungopondereza chifukwa mukudziwa kuti munaba limodzi .america isiye kaye kuthandiza Malawi kwa 10 month kaye tione kuti mulipanga solve bwanji dziko lamalawi
Amalawi ku opa America dziko lopanda yankho pa lokha
America yachita bwano kutelo
Kodi wakuba alindiufulu zopusa
Alibe mphatso yawu president!!
Support criminal adha awa and wina akamati amuvotela😮
Kumkuyu garu wa munthu.
Zozungulira ayi tangoyankhani mafunso komanso palibepo mbalume pamenepo ndi Street thing answer the question pls
Makhothi ake ati,???? Ku Malawi kulibe mathoti anapangidwa Captured ndi mcp ngati injunction ya nankhumwa kutha years nde milandu zinazi anga kambe.. Tinawombera mfiti mmanja...
Guys ma American siwofunika kumawasekelera eya zowona amapereka mathandizo Koma amakhara ndicholinga mudzikomo pamapeto adzakupusitseni then atenge zofunazo mosavuta and we need to know dziko lirilose limene mulimikangano ma American akango yamba kulowelerapo mapeto ake dziko limalowa nkhondo mcholinga azidzapangamo ma businesses azida zankhondo president wa Malawi akadapanda kulankhulapo mukadatiso ndiwogona kwambiri
Chakwera is corrupt,thats why he is defending those people.
Dziko la Malawi limadalira kuphepmpha ku america komweko ndiye americawo awone zochita basi
Galu waluma mbuyache kkkkkk wapenga chakwera
Musavutike ndi kuganizaso chakwera ndi mbava.akanakhara wanzeru akanat America yandithandiza athuwa ndimbavadi
Chakwela ndi. Wakuba. Amange bas mboni ndine
Makhot anthu akugwila ntchito ndi emusip
😂Galu wankota sakandira pachabe.les wait and see. wait
American tsinalakwe chakwelalayo ndiye wakuba kwambili mbava dzokhadzokha sitikumu funa pamozi ndi kunkuyu achoke dpp boma 2025 tatopa komaso joice banda usiletu kunamidza athu komaso athu muchenjele Joyce anaba ndalama ya ndege anayda yekha ndiye chenjelani mudza wona mavuto ngati womwewa komasotu Joyce banda alinali ku mcp motelo idzi akupanga dala akupanga akufuna kuti dpp isawine ku mwela akufuna dpp ndi pp pakati akudziwakale kuti mcp ndiyo winawina kale chonde amalawi musapange mistake kawili Joyce ndiwo tsokonedza my name is Patrick form South Africa
Makondela inu koma akanakhala azipani zina bwezi mutamanga kalekale
Kodi kumkuyu mmutu mwake mulimzeru?
Sizikugwilizana watsala iwe
kumkuyunso ali limodzi muwumbsva
America sadalakwitse ,manyumba mwathu,tikaona kuti mwana wathu akuba,amasalidwa ndi abale amakolo Ake kuti asabwere kunyumba kwathu, chifukwa Cha mbiri yakuba,ndiye dziko Lili ndi anthu akuba ndye ma mericans asekere zupusazo?
Eee achita bwino pule akwiya
Koma abaalee 😂
You are not honest Mr President, kutha mau chifukwa aletsa mbava kulowa dziko lawo?? Mr President mukanakhala wina mukanauza a ma court athu azifulumiza milandu osat mpaka 4yrs milandu isanathe. Munthu womvesa chisoni Chakwera.
Akuzengeleza kuzenga milandu chifukwa chani